Email a copy of '120 MRA, Malawi police officers raid Kamlepo's house' to a friend
Loading ...
Email a copy of '120 MRA, Malawi police officers raid Kamlepo's house' to a friend
Tobacco farmers in Limbe have started off on a good note as the leaf fetched US$1.50 soon after the opening...
kamulepo ndimunthu wamkulu(cars are not kept in houses plz)
Whatever the case, nobody from the Northern part of Malawi will ever be elected for Malawi Presidency. Tikudziwa kuti Kamlepo akulira coz akudziwa zenizeni and is feeling pain of the fact. Everybody has the freedom to cry either in public or in private. Of course chilungamo ndichowawa BUT what else could you do?. Numbers are in the South and Centre.
Revisit your behaviour towards people from the other regions of Malawi otherwise just live positively with the status core for there is nothing that will change it.
Kamlepo, ukudabwa chani?. That is rule of law at its best – osamachita makani mukudziwa kuti simuchedwa kulira. Zisamakomere mbuzi kugunda galu, koma galunso naye akagunda mbuzi zinthu zidzikhala chimodzimodzi.
Stupid are those that sympathize with an empty bucket like Kalua
Shame on you
What about arresting Chaponda for theft of state funds?
Koma abale ine ulemu ndipereke kwa kamlepo, Kamlepo inu ndinubachikuliledi iiiii, pokha polimbana ndi Kamuzu aaaa ndinu achikulile. Panopa muli MDI masapota Ife, osadanda!
Some people commit crimes. When arrested or investigated they claim that they are being persecuted. No one is above the law. Not even Kamlepo vocal or not. What I have seen is that a handful of people just hate DPP. They just focus on negatives no matter how the positives outweigh the negatives. DPP please continue those numerous development projects. People in the villages know the good things you are doing. In 2019 those projects will yield political fruits. Mark my words. Lolani ntchito za manja anu zikuchitileni umboni.
Kodi a boma mufuna kubwezera zomwe zidachitika kwa Chaponda { Kaloswe} kuti
zichitikenso kwa anthu ena osalakwa kuti nawo achititsidwe manyazi? Ngati ali
olakwa, ziwoneka, ngati ayi ziwonekanso. Kodi you have targeted Kamlepo
poti adalinawo pa Kafukufuku wa Maize Gate? Ndiye mukumufunira zifukwa?
A Kamlepo, inu zanu pheee! mtima m’malo. Ngati pali cholakwa, chiwoneka.
Kodi ndale zosakanazi bwanji? A Intelligence athu akungochita inter-party
intelligence, koma ya international yikutivuta.
DPP should tread very carefully. You will start a civil war. It starts like that. When we people are tired they will fight back.
Morally bankrupt President, Morally bankrupt MRA Morally bankrupt Police
Mose muli vizereza mpaka 120,mose mfwenge pala mukulimbana na kanulepo kalua,akayamba ndale achali mu choko uyu,akalimbana na kamuzu so what more uyu mthali wambula mino tungwa .