Email a copy of '15 Lilongwe University of Agriculture students arrested for shoplifting Malawi Gin bottle' to a friend
Loading ...
Email a copy of '15 Lilongwe University of Agriculture students arrested for shoplifting Malawi Gin bottle' to a friend
Rainbow Paints has boosted Southern Region Netball League by launching the sponsorship to the tune of K4 million after OG...
It is sad, the only time University students behave is when they are looking for employment.
Guys palibe nkani apa. Why debating such a petty issue. Anthu amanyamula ndalama mumasaka ku Kapital Hill palichani pano. How do you equate that with a bottle of gin. Thats loughable. Why dont just ask the students to pay money of gin which is not even equal to Mk2000. Anthu akunyamula mabelu andalama mubomamu, ife nkumankangana ndi nkani yoti kwabedwa botolo la gin. kkkkkkkkk kaya zanu zimenezo
one thing that startles me is why the police arrested the other innocent people who were JUST sitting in the lorry, and some who were failing to jump out and run for their lives!! wher is the proffessional of the police there.. nkukawatsekela ndikumawamenya ku m,a cell-ko.. that aint on!! after all guy-yo analibe dollar, ndiye plus ka ludzu after kumenya game yokhwiya heavy… akanatani mnyamatayu??? kk
hahahah….ndi dolo….kutuluka nayo mpaka?………..in fact palibe umboni kuti anaba coz tikamatuluka timadzera pa ma til,pomwe timaperekera ndalama,…so somebody may think anapereka ndalama
I think being at university doesn’t mean u have good manners or ur intelligent no! These kids anazolowera kuba so they wanted to use force. A police nanu u could have changed them wit aggravatd robbery maximum life in prison ena atengelepo phunziro
my mesho ngati one ov d victims, is complaining ov being severely beaten by officers while in custody.
That was good. Mmayesa inu mumakwapula ng’ombe ikakoka ngolo as part Animal Science student practicals. Just drink kachasu ku Mitundu osati za ma “grand theft” ginoz.
Mukumatipangitsa manyazi ana amakhule mbuzi inu mumati udolo umenewo kkkk abakha
this story has been wrongly reported…i was there kma this is not wat happened……u are nt proffesional ase
Alekeni ana
pali nkhaninso pamenepo, malo moti mumange kasambara mukamape botolo la gin asiyeni anawo