Email a copy of '700,000 households in need food assistance: Malawi govt, WFP launches relief operation' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

6 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
Stanley
Stanley
9 years ago

Punish him. He must cry in Lomwe.

Nkhombokombo
9 years ago

Inu WFP kaya mmati ndani! Ife mungotiphunzitsa kalimidwe kabwino kuti tidzikolora zambiri, basi mwatitha! Chifukwa chaka chilichonse mudzingobweretsa chakudyachi.

Angozo
9 years ago

Gogo nditanena kuti ndiwe mfiti ndiyesa sindilakwitsa, munthu wa mtundu wanji iwe ngati iwe ukudya kunyumba kwako usayankhule motumbwa. Ndikuuze kuti sibwino chilichonse kuchilowetsa udani kodi ukuganiza kuti zivute zitani APM angavutike? Wovutika ndi abale athu iye ndi wolemela kale.

SimpleMind
9 years ago

20 years ago my village compound had 12 people including children, with enough fertile land to feed us all year round. Now there are a total of 38 people.

Isn’t it time we addressed the real problem in our country – uncontrolled population growth. Limited supply vs steeply growing demand for food (and everything really!).

Gogo
Gogo
9 years ago

Mwalakwisa kwambiri a WFP.Mukanamusiya pitala asove yekha kuti timukutumule bwino.Pamene apa azitama ngati akupeleka ndiyemwini pomwe boma lilibilethu chimanga.Tikufuna uyu pita alire mwachilomwe. A WFP tiganidzileni tithane ndi mbuli iyi once and for all.

Abono M.A.
Abono M.A.
9 years ago

Bungwe lathu!

Read previous post:
Kabwila explains ‘stealing  from corpses’ comments amidst backlash

Malawi Congress Party (MCP) spokesperson Jessie Kabwila  has explained that her comments in relation to the controversial grants the National...

Close