Email a copy of '9 Malawi Police officers arrested in Karonga for alleged pocketing bribes from maize smugglers' to a friend
Loading ...
Email a copy of '9 Malawi Police officers arrested in Karonga for alleged pocketing bribes from maize smugglers' to a friend
Dear Mr. President, Why an Open Letter? I have decided to write an open letter to you because as a...
let’s remove ignorance on this platform. nkhani ili APA ndi maize smugglers . chaponda sizikumulhuza ngat aphwanya lamulo amangidwe basi.
ngat chaponda anaba nayenso amangidwe if there is enough evidence not political propaganda. coz we may waist a lot for compensations
Maize had passed through the two roadblocks, North Rukuru and Kiwe. MDF soldiers are the ones that impounded the maize around Pussi trading centre.
Pali nkhani apa .Peter anamumanga Chaponda ..Wina akufuna promotion ya Ziiiiiiiiiiii.Mulungu azakulangi .Boss wanu womuchosani ntchito nayo mbuli yachabe chabe.Ku Karonga kulibe corruption kupereka ndi kwawo bola wa mphepha.A khoti musaweruze khaniyi ayambe agwire chaponda..Nkhan ni Chimanga basi.Every master has aduty to protect his subordnates .Ndiye apolice ndi agalu kulimbilana mafupa..DPP aba abaso inu yopepha akukumangani
God, the best judge, may you arrest Zambia maize deal thieves. A Police amangana okhaokha, awo akuwalephela kuwamanga, hence, ife tikudalira inu Mulengi wa zonse. Muli ndi maonyolo ambili omangi iwo ochimwa. Teloni Yawe.
A POLICE KUGONA !!
TULO TOO MUCH
KAMANGENI CHAPONDA
UKO—-”
TAONANI ZIKUKOMERA GALU KUGUNDA MBUZI
if we have a honest government let them arrest Chaponda!
A police kumalizana ntchito nonkha nonkha.Head must protect his junior in the system. Pali border pa RUKULU or KWIWE.Is there ban that say do not take maize through Rukulu or Kwiwe..Bwanji Chaponda Peter sanamumange .Inu kumangana za ziiii ,anzanu atenga K10,000,Chaponda atenga K200,000,000.Ndiye Upolice ndi mbola.