Email a copy of 'Angry father demands justice for son battling for life after Reds violence' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

108 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
mxolisi lukhere
mxolisi lukhere
8 years ago

dzili busy kumenya macivilian m’malo mokateteza nyanja akutibera matanzaniayi!!!!!!!!!!!!!!!!!!!

Kangaroo-Court
Kangaroo-Court
8 years ago

Onsewo muwapititse ku Darfu,akakhale kutsogolo kwa nkhondo.akufuna nkhondo nang si kuno akungogona nkumangdya basi,DRC ikuwayembekeza amenewo,le them go there plz.Asasamba achabechabe,kuipa mtimaa choncho ngati ndinu adziko lina bwanji?Boko halam mukuiyambitsa poyereyera,oskalimbana kapena ndi Tanzania bwanji?

Ndakwiya nanu!!!!!

Sipidy
8 years ago

Kodi amaona off-side ndi ndani? Referee kapena linesman? Oyenera kumenyedwa anali ndani?

mussa
mussa
8 years ago

Stupid soldiers!alla naires,ur masa poes!

GERARD
GERARD
8 years ago

Ma solder apamalawi kuzikonda sichina chifukwa cha kusowa kwa mifuti kumalawi amaona ngati poti iwowo amagwila mifuti ndiye ndiwopambana agalu

fred liwonde
fred liwonde
8 years ago

What iz the role of soldiers in acountry?is it playing futbal ,singing at the stage ,drinking beer ,stealing &what beating innocent people when they want to win the matches in the local futbal pitch?nonsense ufailed to play ure trained game with tanzanians taking part of our land•but busy beating civilians shame on u•if this is what uwent to training for well done u are doing alot•but if not godforbid and what poor management cashgaters like u •organise ure own army league not this with locals or can we call boko harram for friendly with u or we do it ourselves… Read more »

Ine
Ine
8 years ago

Asilikali ayambitse league yawo, azimenyana okha okha.

ndamva chisoni
ndamva chisoni
8 years ago

geofry akuoneka kuti ndi mwana wabwino
bambo a geofry tengerani a sulom ndi anyamata a army onse ku khothi
palibe amene ali pamwamba pa lamulo
get well soon boy

mjiba
mjiba
8 years ago

suspend the team for the entire season not what you have done. Remember the concerns raised at SULOM AGM about having officials from military dominating SULOM official positions this is what you get injustice

Ntepere 2by2
Ntepere 2by2
8 years ago

kugwiritsa ntchito mphamvu in.a game of football ,ofunika tikuitanireni boko haram

Read previous post:
Sulom whip Red Lions with K3.6m fine: 8 players suspended in Malawi Super League

A tough punishment has been meted out on Red Lions for violent conduct during their Super League games against Surestream...

Close