Email a copy of 'APM campaigns for his 'replacement' in Thyolo East' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'APM campaigns for his 'replacement' in Thyolo East' to a friend
Archbishop Thomas Msusa of Blantyre Archdiocese has clarified on why the late Fr. Danasiano Kunkeyani was buried at Limbe cathedral...
baby iwe ndiye uiti wabwera liti dziko lino ukulidziwa komwe linachokera iwe samala ndimalankhulidwe ako ngati ndiwe mulomwe dzako izo
mbava za DPP convoy mpaka galimoto 40 koma yaaaa kuwononga dola zathu za misonkhoooo
Zazii,wa opposition nde angamanidwe chitukuko,kusankha munthu ophunzira sikwabwino et,mesa wa opposition yo amakhala kut ali m’boma kale,cjimasiyana ndi chan,anthu aku Thyolo pliz sankhan wa independent kumeneko asachite kukupangiran zochita,chisankho chili mu mtima mwanu
Koma ashado akewa malaya akuchita kukhulumba, mutuwo ngati chikula mayembe koma kupaliament ko akayankhulako , kamwayo ngati afuna aziti,moseliwa khanyenekikikikiki.
Kkkkkkkkkkkkkk!! Ku nyasa patala plasdent walomw koma kuli anthu owoneka bwino kumeneku ku tyoloku
MUST was shifted to Thyolo by your arrogant brother. There is nothing you did for that constituency save for what your brother did.
Koma ndiye APM anthu ena mumadana nayetu.
Yesterday, I saw the President’s convoy coming from campaigning in Thyolo and it was one of the longest Presidential convoys I have ever seen. It was probably 1.5 to 2.0 kilometres long. Much longer than any of Jb’s convoys. Literally hundreds of vehicles.
They say the more things change, the more they remain the same.
It appears once power is tasted, all values are thrown out of the window!
Convoy ya president imathera pa galimoto ya polisi imene imakhala pambuyo. Enawo amakhala ongolowerera kuti ayende nawo mwachangu. President Arthur Peter Mutharika amayenda ndi magalimoto khumi basi.
Kanyani ndiwe waboza, ine ndinalikonko, anali ndimagalimoto ochuluka zedi, kuposa 20.
Musatinamize apa ngati mumadya limodzi ndikutionongera misonhko yathu.
This guy is so tacky are those notes in his right hand?????
Yes DA that is what he is saying. Oh and he is also hitting the point home that, if you are not an MP of DPP, the gvt wont help you develop your area( or hear your peoples concerns) no matter how ligitimate they are. And we wonder why the NORTH is taking matters into their own hands and why there is the “us and them” syndrome in Malawi. Thats is straight from the head of state!!