Malawi needs a Malawi day twice a week if things are going to change.
Akungolonje
8 years ago
Ndiye zachiMalawi zimenezo pakuti ndi zodula kwambiri a Malawiwo maka ma civil servants azizipeza bwanji poti ndalama ndiye mwaikhwefula a Pitala, ma salary kuonjezera ngati momwe mzanu Joyce amachitira njeee!. Za mkutu basi, mwasowa zonena a President.
Alangizi nanunso ndiye mbatata zenizeni za anthu,….. Kuteroko mmati mwamulangiza zaphindu mzanuyo?
Chengolopiyo
8 years ago
Kodi kachasu ndi illegal brew mpaka lero? Komatu zibwana zimenezo. M’mene amakomeramo!
Chengolopiyo
8 years ago
Finally!! Malawi is waking up to the importance of promoting local products. For centuries we have fallen for junk from abroad simply because it carries labels that are said to attract social recognition and prestige. Komatu tsopano mutiuze kusiyana kwa foreign products produced in Malawi and real indigenous ones. Chifukwa ine chaka cha mawa pa 18 March sindidzamwa Carlsberg koma kachasu wofululidwa ndi anganga anga kunyumba. Kodi kachasu is still illegal brew? Komatu zibwana zimenezo, m’mene amakomera kachasumo!
wo
8 years ago
Malawi imene achina chaponda amati anachoka kunja ku United nations ndikubwera kudzathandiza dziko lawo mmalo moyamba full time businesses. They came with nothing just like pitala and they want to suck Malawians.
Bwampini
8 years ago
Fodya eti misala
bruce munthali
8 years ago
Mutharika Day!
GVH KHOMBE
8 years ago
Why can the be be celebrated on world heritage day? Other countries like south Africa do the same
Myao
8 years ago
And yet he donned a Eueopean suit, at least dzitenje or dzikoka za chingoni wouldve made sense.
Look at his govt, always happy to contract foreign firms at the expense of local one and there he is telling us to act to the contrary, koma abale.
Malawi needs a Malawi day twice a week if things are going to change.
Ndiye zachiMalawi zimenezo pakuti ndi zodula kwambiri a Malawiwo maka ma civil servants azizipeza bwanji poti ndalama ndiye mwaikhwefula a Pitala, ma salary kuonjezera ngati momwe mzanu Joyce amachitira njeee!. Za mkutu basi, mwasowa zonena a President.
Alangizi nanunso ndiye mbatata zenizeni za anthu,….. Kuteroko mmati mwamulangiza zaphindu mzanuyo?
Kodi kachasu ndi illegal brew mpaka lero? Komatu zibwana zimenezo. M’mene amakomeramo!
Finally!! Malawi is waking up to the importance of promoting local products. For centuries we have fallen for junk from abroad simply because it carries labels that are said to attract social recognition and prestige. Komatu tsopano mutiuze kusiyana kwa foreign products produced in Malawi and real indigenous ones. Chifukwa ine chaka cha mawa pa 18 March sindidzamwa Carlsberg koma kachasu wofululidwa ndi anganga anga kunyumba. Kodi kachasu is still illegal brew? Komatu zibwana zimenezo, m’mene amakomera kachasumo!
Malawi imene achina chaponda amati anachoka kunja ku United nations ndikubwera kudzathandiza dziko lawo mmalo moyamba full time businesses. They came with nothing just like pitala and they want to suck Malawians.
Fodya eti misala
Mutharika Day!
Why can the be be celebrated on world heritage day? Other countries like south Africa do the same
And yet he donned a Eueopean suit, at least dzitenje or dzikoka za chingoni wouldve made sense.
Look at his govt, always happy to contract foreign firms at the expense of local one and there he is telling us to act to the contrary, koma abale.
Fodya eti