Email a copy of 'APM says no good relations with JB: ‘If she calls me, we can work together’' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

97 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
chindungwa jnr
8 years ago

Onsewa ndi mbuzi zokha zokha palibe wabwino. Kuba,kupha,kusowa mankhwala mu zipatala, umphawi sungathe ku Malawi chifukwa atsogoleri saopa Mulungu

Denguzman
8 years ago

For her safety, let her stay abroad coz achanganya awa a DPP sizocheza akafuna kuzimitsa munthu iwowa sachedwa moreover ngozi ya lorry pa Kanengo angayiwale ndani mmalawi muno. God be wit u JB and we wl kpon praying for ur safety.

Ntata boy-BT
Ntata boy-BT
8 years ago

musathamangire kutukwana this Ntata man has a lot to reveal lets listen to him first

GRM
GRM
8 years ago

I am glad i am not a member of a party whose President is a run away cashgate suspect. Lutepo ali ndi umboni onse. Amalira Savala mukhoti lero.

Chifi Jasitasi
Chifi Jasitasi
8 years ago

If Amayi is clean why can’t she come home?Everytime she is lying to us that Pitala is keeping a small pistol in an Olive branch as she learnt from her deceased Arab friend Yasser Arafat.Mmayiyu akudziwa kuti Malawi yachema ndinkhani ya cashgate ndipo akuinikikira patali.The moment she lands pa Kia azamumveka nawo unyolo.Akuona ngati amalawi akuyisekelera nkhani ya azinzake Lutepo ndi Mphwiyo?

Tione
Tione
8 years ago

Mutharika ndi galu weniweni. Mbuzi mano kunsi, nkhumba ndipo kanyimbi. Misonkhano yake amati ya chitukuko koma nkhani ndi JB basi. Stupid and dull minds discuss people while clever and intelligent minds discuss ideas. This man Mutharika’s days are numbered. Akatsegula pakamwa pake ponyansapo zotuluka ndi zautsiru zenizeni. Vuto ndi anthu a kumidzi osadziwa. Amangoti poti ndi mng’ono wa Daniel Phiri basi tisankhe yemweyu. Malawi is not a family estate.

jazila chigwenembe-Balaka

Who calls who?to where?why?
if Banda has a case to answer let her do so.if she is free let her go.release her benefits and whatsoever.pay her as per law.you can’t work together because you don’t march feathers.you are all malawians.

Chawanangwa
Chawanangwa
8 years ago

So most of you stupid people want JB killed?

kaliyeka kudandaula
kaliyeka kudandaula
8 years ago

dziko lakuvutan ili malipilo sakuoneka ndalama zathu kulemera nazo..ana anu ma xul odula kwa basi..mot mkonzeso tsogolo la anzawo ana anuwo..mwaiwala kut ana anu akadzalemela azidzawabera ndiomwewo

MAYE
MAYE
8 years ago

I think Mama was supposed to come back home if we are to agree that she has a clean record as far as cash-gate is concerned. The more she run away from home, the more we think that she was connected somewhere. I feel that even if she can be prosecuted, she will come out clean ngati sizikumkhuza. So come back mama. This is your home, we need you

Read previous post:
Blantyre City Council sends Kasunda to Connect Summit in Tanzania

As part of its continued efforts to turning Blantyre City into a Smart/Digital City, the Blantyre City Council is participating...

Close