Email a copy of 'Atupele home robbery: Malawi Police arrest three suspects' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

19 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
kwalewera
kwalewera
9 years ago

Would like to commend the police for a job well done. However would like to join the others who have observed that the police can not act with such speed when ordinary Malawians face the same fate. There are Many Malawians who have been robbed motorcycles, computers etc but have lived every day with high expectations about the recovery of there goods, alas nothing has come forth. Police please note you are paid from tax money paid by even the so called ordinary Malawians. Remember the book animal farm. Wake up for God had observed these things for too long.

Nat
Nat
9 years ago

Will the authority do the same to anoone like me. .za ife sizipezeka

MELINDA
MELINDA
9 years ago

kumavutitsa kubela anthu usiku, m’malo moti muzikathana ndi azibambo omwe amumanyamura azimayi a BOKO HARAM (MAHULE) ogawa matenda.kupusa

Tman
Tman
9 years ago

Ndalama mumasunga mnyumba zambiri aung’ono-ung’ono, mukati musunge kubanki ndiye mumakasunga ku ulaya. Kukuberanikutu sichina ayi; gapu ya pakati pa anthu olemera ndi osauka yakula kwambiri. Ndipo ndikanakondwa akuba amenewo ankanati azipanga ngati Robin hood. Makamaka kwa inu anthu andale, mukutizunza a malawi ndinu anthu oipa , mbava zikulu-zikulu. Mukaba simukusegulanso makampani kuti tizipeza mwawi watchito. Zoona ndithu maofesi anu ndi a mmaburigikesi -ZIMANDIWAWA

Tunthumbwana tambewa
Tunthumbwana tambewa
9 years ago

Pankhani mwina ndayiwala koma ndidawerenga ngati munkati atupele adalibe ndalama only 35000 idali muwaleti lero mukuti bandles of cash moti 35 ingakhale bandles? Komaso wallet yolowa 35000 ndiye ndi yabwino.

Babalu
9 years ago

Zigawenga zimenezo muziphe tatopa kukhala mwa mantha mdziko mokhala mwathu

Zanga Phee!
Zanga Phee!
9 years ago

Why not showing pictures of robbers we know Muluzi editors please watch these things are you in favor of the robbers perhaps See my name.

victim Chamkhuni Lwazazi
victim Chamkhuni Lwazazi
9 years ago

As usual I commend Malawi Police for the job well done. i wish such efforts were not only for ministers and high level people in the society. The police should not neglect, ignore and off course connive with criminals when cases are reported by ordinary citizens. Please, please, please Malawi Police we pray that you keep up with good sacrificial efforts to net all these BAD people in our loved country. These caught know most of their friends!!!

ine
ine
9 years ago

A Imran; mwatiyipitsira dzinatu apa.

Yankees
Yankees
9 years ago

Koma Atupele Tayo imakukhala ngati asokela pompo mwana wa mjomba Atupeelee! Adakutsukuluza mafanatu awa saizi yako mwana mjomba amangwetu!! Koma osamachita zija za mdala wako zoti kumachangamuka pa Tawoni ayi, komanso kunyumba kwanduna amlawi kopanda apolice at least 4 kuti enawa akabuleya ena alert mesa amatelo kwa azathuku? Nduna mudachepetsa move yaboo, mukukawachepetselanso chitetezo mkuwapatsa ma Gad a G4 siumbuli umenewu?

Read previous post:
Times TV Suspends Blak Jack for soliciting ‘bribe’

Times TV has suspended dancehall star cum TV presenter Blak Jack on allegations of soliciting a K20,000 bribe from the...

Close