Email a copy of '‘Beware of gossipmongers’: Thyolo chief advises Mutharika against breaking ranks with VP Chilima' to a friend
Loading ...
Email a copy of '‘Beware of gossipmongers’: Thyolo chief advises Mutharika against breaking ranks with VP Chilima' to a friend
Archbishop Thomas Msusa of the influential Catholic Church in Malawi who led a memorial mass of late president Bingu wa...
fumu ya mahala ndawonelepo, vinyake tilumbengeko, apresdent velani ulangidzi wabwino. akulu akulu ndi mdambo modzimira moto.
yayaya malawian politics eish
Mkanakhala ine Mkanasitha, iwe mpaka kuyamba kupereka mgawanitso. Shame on u. Leave the intellectuals to utilize their brain vision.
Mbuzi
Mfumu ya nzeru imeneyi
when it comes to issue of VP, let the president decides who to work with. in Malawi we vote for the president not the vice infact we should amend our constitution to allow the president to appoint and fire the vice president at will. What we have now is all wrong and zimakulisa mtima vice president knowing kuti sangachisedwe. Secondly my humble advice to the incumbent VP and those to come is that it is not a must that Vice presidents should succeed to power no. Ndiye osamakula mtima apa ayi.
Wish all the chiefs were like this one. Other chiefs, please buy a leaf.
AMwene wa Mwene Ngolongoliwa – wisdom of ages. I am proud of you. We are one unifying the nation.
If this is the only Lomwe chief enawa ndi ndani? Kutengekela zaweni. pezani wanu mtundu osamangoti lomwe lomwe. If you do not fall under ngongoliwa you are not lomwe
Mafumu anzeru osati mbava zinazi zongodya ndalama zamalo