Email a copy of 'BT United rejects Silver claims on signing Limbani' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

19 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
nyasi mmaso
nyasi mmaso
9 years ago

That’s why ine will never suport bullets ana amasiye koma opanda ulemu. Kwawo ndi kuba kutukwana kupempha. Team mpaka season ikupempha? Enafe tikungosintha sponsorship ngati zitenje za mkazi wa mimba.

Danga Lapezeka
Danga Lapezeka
9 years ago

Typical of Malawians,Jelousy with other peoples success.Mupwisa utsi chaka chake ndi chino Bullets simungaithe ,ilibe anzao pa Malawi pano. Koma mukapitiliza inu a SECRETARY A SILVER TIKUCHITANI TINTINI MUMVANSO.

Ineyo
Ineyo
9 years ago

Utolankhani wa mike bango ngoseketsa heavy kuulutsa nkhani b4 investigation…..atolankhani ongowatola mmakwalala….MIKE BANGO WA SILVER UNYERA CHAKA CHINO IWEEEEE

Alick Prescott Makanjira
Alick Prescott Makanjira
9 years ago

Silver is jealous of Bullets’ recent exploits. You thought you are the best club on the land to the extent of refusing to sell your players to the people’s team.KhKKKKKKKKKKKKKKKKK! Whatever the case, you will never substitute Bullets mpaka Yesu adzabwera

victor Limbani
victor Limbani
9 years ago

Ndati ndiyankhepo pa nkhaniyi!!

Ine ndine wa Bullets,silver isakunamizeni kalikonse.ma fon Nde akumaimbadi Kuti akundifuna koma ndawauza Kuti anachedwa.andilonjeza zambili mpaka galimoto,koma mtima wanga ku silver sindingamenyeko mpila.the Only team in Malawi Where I can expose myself is Bullets!! So Silver GET OFF!!!!

Peter Benga
Peter Benga
9 years ago

Inu a silver lero muwafuna anzanu.suja pa dzana paja munkatumwa ndi chawanangwa wanu uja.Nanunso mwayandama mu thobwa

Ken Malinda
Ken Malinda
9 years ago

Noma ikumagula maplayer okalamba , chule Wadabwa ,James zakazaka, mwinanso Gilbert Chirwa

ackim maulidi
9 years ago

silver yapenga kkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkk

Mbunama victor
9 years ago
Reply to  ackim maulidi

live longer manoma let them talk bcoz they are poor due to their thievery activities when money is given to them

Yankees
Yankees
9 years ago

Anakoma mateamuwa amusiya Limbani, tione mwina mugulitsa kuti? Tangotchajani ena akupaseni makobili, Limbani is not a Nomber one player in Malawi, Eh kulimadolooo!

lakwathu
lakwathu
9 years ago

A Malawi sindife opusa kuti muzitinamiza. Ma club Mwaonjeza kunena mabodza and u r losing ur credibility

Read previous post:
Malawi Music Awards to honour Sauka: Composer of National Anthem

Composer of the National Anthem late Michael Fredrick Paul Sauka will be honoured by the organisers of  this year’s annual Music...

Close