Email a copy of 'Bullets get revenge on Wanderers: Malawi TNM Super League' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Bullets get revenge on Wanderers: Malawi TNM Super League' to a friend
United States embassy in Lilongwe granted 115 visas for Malawi delegation to United Nation in New York, confirming that the...
zimatere zimatere bwenzi zikoma kudu kudu kudu ng`omatu zimenezo
Comment # 69 – Eee ndimmene zimakhalira kodi eti? Ayi tamvera inu. Nde mukatero sing’angayo mumampatsa zingati? Mwina nafenso tingapite konko tidziluza nawo. Komabe ife a BB tilibe nthawi imeneyo ife wathu ndi Mulungu (Yehova) osati mafano (Baal) anuwo. Ndipo mukanakhala kuti mankhwalawo akukupindilirani bwanji osaigaira Flames idzatengeko World Cup? More fire BB.
pepani a Kananji,pepani a Nyamilandu,pepani a Madeira,pepani a Yona,pepani a Zidana,pepani a Melvin Nkunika ndi nonse anafedwa,chapha malemuwa ndi thiraki yonyamula clinker ndiye malirowa palibe kuona nkhope coz sikuoneka nkomwe. MAULE amapamantha zedi ,aliponso wina?Tinanenatu paja kuti 4-0 ya Al-Hillal ija munya nayo nonse kuyambira iweyo neba lero siizi? Pali mau,ngati sukumvetsa kachotse BB pa # 1 ubwerepo iweyo
Zinthuzi zikuwoneka ngati zazing`ono, palibe wa manoma amene anapita kwa ayaya.
amene anapita kwa msing`anga ndi a MAYI MOFFAT ,Mzimayi wa ku Lilongwe uja amati Manoma akawina Carlsberg avula uja.
A Bullets akumaika mankwala mmagate olowera mu stadium , komanso amalemba mayina onse a maplayer a timu ina mkupita nawo kwa msing`anga kumene msing`angayo amawamanga miyendo ma playerwo ndikuwapatsa chidima kuti asamawone bwino pagolo., ndipo amawauza kuti mainawo akawaike pa centre poyambira mpira.
kunja kuno kuli Mulungu mudzafa imfa yowawa takudziwani.
M’ngoni weniweni nawenso wasanduka ref? Osangovomera kuti NEBA waluza. Mumuwuze Yona wanuyo kuti asiye zomabetcherana maphokonyorewo. Ameneyo ndiamene akukupweteketsani. Maulee Woyyyyeeeeeeeee.
ine kumva yogati nthupimu, wishing i ‘d b there 4 myself to celebrate with timu ya mfuko.
Manoma mwafa basi mukabweze ngongole kwa Ayaya kuti muyambe kuwina ndiye poti ndinu osamva mukhala choncho
Brava maule
Moni moni moni a Elia Kananji.Kaya mukumva bwanji mthupimo?
Bravo maule zangoonetsa kut neba ndi amene amayambitsa ziwawa akuluza, ife tinaluza carsberg kma anthu sanagendedwe