Basis musipilila a bb ndalama zopempha ndi choncho
wolangiza
9 years ago
zowonadi munthu akamachita bwino ambiri samufunira zabwino .tawonani apa amariwongo angokamba za BB mumaro monyadira BB kuti yikusangarasa dziko la marawi .chifukwa pa malawi palibe timu yozipereka pankhani yamasewero .ndiye wina ungoti nyoooo uyerekeze uwone zomwe anawona azako ku nsanje
Lloyd Matambula
9 years ago
People we are all Malawians lets support BB bez this are international games. They are carrying Malawian flag……………………………………..aaaaaaa!!!!!! shame on you
zanga phee
9 years ago
Mungoti mukufuna ndalama , Kodi game ya Saturday munapeza ndalama zingati, tiuzeni mwachangu, kumangodalira kupempha basi , neba zanyanya tsopano.
chilombo
9 years ago
Koma Bullets nditeam yosauka guys,kupempha ngati amaskini. Game iliyonse tizisonkha?
Phodogoma
9 years ago
Kondie Msingama is likely to be a poor mathematician or he is a trickster who steal in broad day light. I mean how does he come up with figures for CAF? Who is his accoutatant? Shame on you Kondie. He estimated 30 meter for the trip to Comoros. Now he is estimating only 12 million for a trip to Sudan. I expected him to mention around 100 million. Unfortunately if you give them 12 million what you hear tomorrow will be that the guys have left by bus as they will board a plane in Uganda.Dribbling of this kind can… Read more »
bb ipita
The Fombon game deserve to cater that little amount to fulfil the trip to Sudan koma basi mwaba dollar zija. BASI khalani musapite. mbava
Amayo munaziyambilanji mulibe ndala kupempha mpakanaliti mukakhale Ku ofanikeya muzikalandiranawo chithandizo chochokera mmabungwe akunja
Wasanje utopa wenkha BB ipitiriza kupanga bwino ngankhale tipezane ndimavuto poti pamene pali Mavuto mtendere ukubwera dikira uwone tikunyamula Caf mumalere iweso uzankhala woyamba kusangalala
Basis musipilila a bb ndalama zopempha ndi choncho
zowonadi munthu akamachita bwino ambiri samufunira zabwino .tawonani apa amariwongo angokamba za BB mumaro monyadira BB kuti yikusangarasa dziko la marawi .chifukwa pa malawi palibe timu yozipereka pankhani yamasewero .ndiye wina ungoti nyoooo uyerekeze uwone zomwe anawona azako ku nsanje
People we are all Malawians lets support BB bez this are international games. They are carrying Malawian flag……………………………………..aaaaaaa!!!!!! shame on you
Mungoti mukufuna ndalama , Kodi game ya Saturday munapeza ndalama zingati, tiuzeni mwachangu, kumangodalira kupempha basi , neba zanyanya tsopano.
Koma Bullets nditeam yosauka guys,kupempha ngati amaskini. Game iliyonse tizisonkha?
Kondie Msingama is likely to be a poor mathematician or he is a trickster who steal in broad day light. I mean how does he come up with figures for CAF? Who is his accoutatant? Shame on you Kondie. He estimated 30 meter for the trip to Comoros. Now he is estimating only 12 million for a trip to Sudan. I expected him to mention around 100 million. Unfortunately if you give them 12 million what you hear tomorrow will be that the guys have left by bus as they will board a plane in Uganda.Dribbling of this kind can… Read more »