Email a copy of 'Bullets players now focused for ‘more glory’' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

15 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
Isaac B. Fungulani
Isaac B. Fungulani
8 years ago

Mwaitha kwabasi maplayer bcoz amangofuna kukolora pamene sanalime. shame to u big fish(masapota)

AKIJA
AKIJA
8 years ago

Dzikomo ma prayers we love u all Guys .

Crisiano
8 years ago

Thus Hw The Peoples Tim Iz

Thakwalakwa
Thakwalakwa
8 years ago

Bullets players need to be commended. You are Champions.Donnot be disturbed by these opportunistic supporters.

Ife timadabwa kuti kodi chifukwa chake mumalimbilana MAUDINDO. Tamagwirani ntchito inu ma supporters kuti muzithandiza team OSATI kudyera Maplayers.

Zikomo Ma PLAYERS kuti mwaonettsa kulimba mtima osamawaopa masopota samenya Mpira. MUMABVUTIKA NOKHA NDI TRAINING KOMANSO PA GAME.

Lovemaniac 91
Lovemaniac 91
8 years ago

Ok, let me c outside. # feels gud to be back in love!

Alpha songazaudzu
Alpha songazaudzu
8 years ago

zilibwino

KUKAYA WA KUKAYA
KUKAYA WA KUKAYA
8 years ago

ONSE OKHUDZIDWA NDI CASH GATE KU STADIUM ASAPASIKESO MPATA KUYENDETSA TIMUYI MWANJIRA INA ILIYONSE.

MBAVA ZONSE KWAWO!!!!!!!

Blessings Kaweru
Blessings Kaweru
8 years ago

Anthu osakonda timu ngati awa sakufunika

Chidzukulu
Chidzukulu
8 years ago

Abale mwanyany kutola khobwe. Team ilibe ndalama. Player monse wayambira kukhetsa thukuta phindu lake osaoneka. Alipo ena amapita ku stadium game iliyonse koma kuwafufuza kuti mpira adaonera liti simulipeza. Amangopitila kukaba mma gate basi. Anthu onyansa inu. Kubwezeretsa mpira pansi basi. Stupid!

Aubrey Norman
Aubrey Norman
8 years ago

Basi anthu kumangozolowera kuba malo muwona umphawi wa Team yathu kuti ulibwanji mukufunanso kuyibwezeretsa pansi team otero akapezeka olakwa achoke.

Read previous post:
No apologies, MCP tells Mutharika: Malawi News hits at ‘senseless’ opulence

Malawi Congress Party (MCP) has refused to apologize for its critical comments on President Peter Mutharika on his UN trip....

Close