Email a copy of 'Bullets risk losing Nyasa sponsorship:  ‘Civil war’ in Malawi champions camp' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

34 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
peter spark
peter spark
8 years ago

These guyz eeeeeee sakonda team koma yet ndimabige ateam

amfana
8 years ago

nthawi ya kondi anthu wake ndi womwewa,lipipa ndianzakewa amamusokoneza kondi.lero ayambanso ife ngati masapota takwiya nawo.

Kelvin Milanzi
Kelvin Milanzi
8 years ago

Bullets ndimaikonda bt ma big ake akaona dola mitimayaw sikhala mmalo nde mwina zimawasangala akakhal opanda sponsorship mwin kungowasiy bas

Martin
Martin
8 years ago

A Bullets alibe mwambo. Tangowasiyani, azitolera ndalama mmaget basi. Asatinyase

Oscar D Phiri
Oscar D Phiri
8 years ago

Iwe Neba unazolowera kunkhala wopanda wokuthandiza kuba basi mukukangana ziyani?

NYIX EUEL
8 years ago

Neba hehede!!!zamanyazi osakwanaso chaka, mpite kwakhoswe ubachalawu mpakampakatu.Come to Ngokwe more sponsers than ndudu

Chithumwa
8 years ago

zikutheka tinaku uza zija zosokoneza zija mesa keep it up fire burn amwali

fisher uja ndineyo
8 years ago

Bullets ndi-team yachimidz ndipo inazolowera kuvutika komaso ndiyohititsa manyaz ingowasiyan makape aona zochita

Fikila Peter
8 years ago

Mungonena kuti simunakozeke kuthandiza timu.musachuluse zokamba.

Messi
Messi
8 years ago

Ukazolowela u bachala ndi choncho. Kupeza mkazi, koma zochita zako kukhalabe ngati bachala. Neba kuzolowela ubachala.

Read previous post:
MP welcomes Malawi police budget reduction, says law enforcers must cut roadblocks

Karonga Central legislator Frank Mwenifumbo on Thursday became the lone voice in parliament welcoming the reduction of Malawi police budget,...

Close