Email a copy of 'Bullets to play two Mozambique clubs for Caf preps' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Bullets to play two Mozambique clubs for Caf preps' to a friend
Two Malawian players who play for former Super League club champions Silver Strikers left the country on Tuesday to Mozambique...
haahahahhahaha kodi BB izisewera CAF yokha? Kapena ma player amatimu ena mukufunawo azisewerera BB ku CAF kokha? ngati a BB mukufuna kugula player tsatani ndondomeko yabwino, timu ngati sikugulitsa player basi ndi wawo asiyeni. Ngakhale ku Europe matimu amakaniza ma player kupita ku club ina pa zifukwa kkkkkkkk
ikanakhala mbuzi tikanaidula makutu kuti mwina ingayambe kuva amalawi tidzanva liti kuti nsanje siipindula yakwana nthawi yoti amalawi tisinthe ndichifukwa chake timapangirana nsanje ngakhale kudziko laeni
Eeshhiiiii
lets pry ziyende bullets ndi timu yadzikolonse anthu onse akuyebekezera bullets mu caf tiyeni tigwirane manja amalawi ndizanthuzomwe izi
Kuchulusa zoyakhura a bb mbuzi kkkkkk
Gooo maule azachita manyazi
Amalawi yakula ndi nsanje mmalo moti mulimbiki now ur still to useless even a bb wo atawina mukundiuza kuti that money zingapite ku zambia asi
Msungama and Fote involve your friends. zinthu sizikuyenda coz your attitude yozikonda
Matama achulukitsa a BB
Mr Fote, where were U when Wanderes and Big Bullets sighned a memorundum of not poaching prayers from one another? Were U in Burundi or Algeria, can u say akutikaniza ma Prayer chonsecho u want those other clubs to die completely? Ife timati mwina mudzipempha matimuwo timafunako wakata wakati kodi kunoko tingasinthane ndindani? Munalowa Musanankhozeke? Then just withdraw matransfer akuoneka ngati anvuta awa? Mkazi ngati wakukana a Fote timakayang’ana wina!!! Dont forse a Horse to drink water men!!?.