Email a copy of 'Burundian murder Malawi man, arrested as mob loot his pub' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Burundian murder Malawi man, arrested as mob loot his pub' to a friend
Names of suspects in what is known as Malawi's Cashgate public finance scandal that rocked the country last year as...
man dont let that guy coz mukamusiya nde ajayila..i mean you police give this people two much freedom nde tiziwona coz this is just the beginnin!
malamulo kulibe kuno thus why anthu afika potenga law into their hands, ma foreigners amazunza amalawi, kuwamenya, kuwasekela mu factory, ndalama zochepa, dnt be suprised zinthu ngati izi zikuchitika. the official know all this koma nothing is been done, generation ya anthu oopa ndi ogona inatha. mpaka k800 moyo wapita,,, amene is against what is happening at nchesi aganize zinakamugwela kwa m’ale wake. anthu amenewa ena are criminals. ma refugz & foreigners who r who undocumented do access health services even business opportunities. amakhalanso bho kuposa ife ma citizen. go to mozambique, south or any country muzaziwa koma ku malawi… Read more »
The man is from Rwanda not from Brundi, 20 of these people 1 of them is a Brundi they hide their id because of Kagame plus manyazi a .1994.wakusina khutu ndi nasi.
tsopano mwayamba kulitenga malawi ngat ku brundi et,u must go back to ur fucken country Brundi.
I bet to differ on a call to kick out all the Burundians, we can not brush the entire nation with the same brush for an individual’s ill behaviour. As irrational as it sounds, I fully condemn the killing in general, no one is entitled to take another individual’s life. We need the authorities to see to it that the law is abinded by. remember the xenophobia attacks that broke out in RSA, initially they started by reckless sentiments, and fueled by an incident of a similar nature. In the end innocent lives were lost including that of those of… Read more »
Totally true and humanely. That is how we are supposed to be like
Nthawi yafika ma Burundi onse abwelere kwao kulibe nkhondo sungaphe munthu chifukwa cha 800mk is a big no…then
Ine2 ndinanwna kale kuti Maburundi azipita kwao koma anthu inu simmamva,Anthuwa ndi amwano hvy,kulikose kuli m’bulundi mukafuse anthu akumeneko akakuuzani kuti ndi ovuta,Koma akubomawo ali zimachende phwiii,apa si awa ajaila mpaka kumapha nzika yathu.Pano loko muziti mwamumanga zipindula chani ophedwayo adzuka?Azipita awa nkhondo kulibe ku Bulundi,Rabish my country
Apolisi gwirani ntchito yanu and show your professional
Ma Burundi mubwele ku Mangochi kuno timapanga chakwanu leka funsani a Police pa Mangochi sitiopa futhi timaphiriphita ya manja Mangochi woyeeeee MP woyeeee
Its sad that the fracas ended in death. If the story is true, it raises a number of questions – why did the Malawian want to leave the bar without settling the bill? And indeed, why did he not just negotiate with the bar owner to settle the bill later if he did not have any cash at the time? For Burundian, did he really have to stab someone to death for Mk800.00? Could this be a reflection of the moral decadence of our townships today where thieving and violence are the order of the day? SAD INDEED.