Email a copy of 'Calls to split Mzimba: Malawi’s largest district 'denied deveopment'' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Calls to split Mzimba: Malawi’s largest district 'denied deveopment'' to a friend
Former Malawi national football team striker Russel Mwafulirwa is set to bounce back from a long lay -off after signing...
Tiyambe Kaye ndi federation, otherwise things will remain the same.
This Mzimba issue its not for the government its for the chiefs who are the owners of mzimba . spliting mzimba cant bring development utesi uwo.
Mzimba kunangotsala kugawa DC let it have two DCs nANGA MUKukakamila DC mmodzi ndi chani cholinga anthu azikasayinitsa ma voucher ku Mzimba Boma inu mukuvuta ndi ma night allowance surely i hate the staff at Mbelwa Assembly mukuzunza ma offesi ku North since you demand alot.
Please DEC members tayikonzani ndi chipwilikiti chokhachokha you find the rooom is full of cleaners and passrsby yet senior officers from the North angoyima mxxxxxiiiiiii tigawe DC basi
No way. Malawi should be split first before Mzimba. The North must be a country on its own or become a federal state. Then we can talk of splitting Mzimba,otherwise there is no reason.
Cholinga chogawira mzimba sikuwina mavoti,nchifukwa chani mmakonda kunyoza atumbuka pamene iwo samakunyozani? Achewa komanso ayao ndinu anthu opusa komanso zitsilu zachabe tisiyeni,pamene ankagawa maboma akwanu tcheya eanuyo ndani ankakuyankhulitsani? Zitsilu inu nonse mkulowerera pa nkhani za eni. Your president is failing you still dsnce for him,it shows how dull you are.idiot,dwalf,otomatonz.
Mukagawa into several districts ndiye suddenly mukhala ndi anthu ambiri oti mpaka kuwina chisankho cha president?
Anyway, za atumbuka izi ife zisatikhudze!
Simple. Ngakhale mumgawe Mzimba into ten districts population will remain the same. I propose kuti tatitumizekoni ife a Mihavan tikazigawire malo and you will see a population boom and development. Tikhoza kukachulukana mmene tachulukira ku central more especially Kasungu such that we are second to the Chewas by population, and very soon tifanana nawo kenako kuwaposa. By the way, kodi anganya nkhani yakubediyi amaimanya chomene?
Up to 4,thats absurd, i think just 2 can work or atleast 3,(1)-mzuzu +ekwendeni+enukweni+bwengu & south,Lusangazi,elamleni,Lunjika going west up to chigude,chikhwenge,bala then north to matuli and back towards west ekwendeni (2) the current mzimba central going north to lunjika,south to jenda,west to embangweni up to boarder then north up to mbala chanda then east wards, (3) Euthini with all boader areas (zambia)and east to Ekwendeni, north to Rumphi
Up to 4,thats absurd, i think just 2 can work or atleast 3,(1)-mzuzu +ekwendeni+enukweni+bwengu & south,Lusangazi,elamleni,Lunjika going west up to chigude,chikhwenge,bala then north to matuli and back towards west ekwendeni
Mzimba is just too big a district. Jenda is in Mzimba, Bwengu is in Mzimba, Mbalachanda, Mzimba, Mpherembe Mzimba. No, no, no! It’s time to split it. M’mbelwa is the one insisting not divide the district for his personal interest and gain. Mzimba should not suffer because of a one Chief. You remember some chiefs were selling people during slave trade! Divide it now. Chief chief chief what! Though am currently in UK, i want it divided. Education two DEMs, Health two DHOs, Agriculture two DADOs, is this not enough evidence to divide it?