Email a copy of 'Cancel demo, Beam ‘well-wishers’ appeal: Malawi CSOs says nope!' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Cancel demo, Beam ‘well-wishers’ appeal: Malawi CSOs says nope!' to a friend
"The Interview," the provocative comedy that triggered a devastating cyber attack on Sony Pictures, went straight to U.S. consumers on...
Demo is on madzi akusiyasiya moonjeza and mlakho abweze ndalama za nac after that apm must resign
NGATI MULI ACHISONI NDI MALAWI, WHY NOT RAISE MONEY TO SORT OUT ISSUES IN HOSPITALS, SCHOOLS ETC. WHY RAISE MONEY FOR BEAM WHO ARE ALREADY RICH. CORRUPTION AT ITS BEST. YOU KNOW WHEN U BUY GENERATOR FOR THE HOSPITAL THATS GENUINE WELL WISHING. WHEN U DO IT FOR BEAM THE BIG PEOPLE WILL DO SOMETHIN G IN RETURN. KATANGALE BASI.
CAN MPS PLEASE DISCUSS THIS WELLWISHING BUSINESS AND MAKE IT ILLEGAL. TATOPA NDI MA CHAKUTICHAKUTI GATE.
Atumbuka demo yanu singatheke, believe u me. We had a common cause in the Bingu era, not this hatred based so called Demo. U will believe me! U can not amass the support you are dreaming about- no way! Malawians are more awake this time!
Umbuli ndi umenewo! Politicians sow a seed of tribalistic anarchy sothat they can easily control and manipulate u. Development of Malawi will need all Malawians inspite of their demographics.
The problem of seeking solutions from human beings. There is no one who will bring solutions to our problems other than The Lord. People will be people greed & selfishness. No matter who we can put in government the fact remains the same, these are politicians they will be politicians
well demos or not…but ..nismsnagement &stealing aid money not plausible…oneway to send msg is demos…amebe amapha anthu ndi a boma noe cso….bodza!
Tell BEAM Trust to refund the money be4 January 13th apo ayi Mass Demos more fire!
Stability ya dziko custodian ndi President NOT Csos.
Abwanawo auze amayi kuti alandire thandizo akabweze ku NAC
Demo for male president is better than the against a woman? Iwe Ntambo zija unkapanga mu great hall kumalimbikisa ma Demo ukadali nazobe? Ufuse undule zozuza a malawi and pano he is a born again iwe wangomaliza ku chanco in 2008 and mageyi eeee ma elections ayi koma living standards how can we economically enjoy a cashgated nation? Paja unkapanga BAH sunaphuzire logic kodi? Trapence uchenjere mulili wako wasala pang’ono ask undule! Sikuwopseza koma be guided by your consciousness!
Well! Well!! Kwaaachâ! Malawi oyeeeeeee! Atumbuka nonse muyimike manja tizikuziwani bwino.
Ife ndiye timadana ndi DPP ndipo demo tikapanga nanga tinamepo apa!
he umbuli apa aaaa!demostrations doesnt mean destroying properties.change that mindset kungoloweza chilichose.poti 2011 anaphwanya katundu ndekuti pano azaphwanyaso nde chani..if you dont have ideas nthawi yino njolima…let those who hv this country at heart demostrate..adausi ndi NIB amapanga za HIV/AIDS basi anthu asayankhule.apresident anu amene kugawila atolankhani ndalama za AIDS kuba kunasala k8million ili kuti…aDPP mwayambilaso nkhanza zanu mukuti anthu asamayankhule ngati mwina inu ndi mafumu.awuzen amayi anuwo azikasesa munsewu amayambisilanji bungwe kavunyani wachabechabe alibe kalikose.