Email a copy of 'Cashgate gunshot survivor Mphwiyo allowed to travel to South Africa for surgery' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Cashgate gunshot survivor Mphwiyo allowed to travel to South Africa for surgery' to a friend
Malawi Police has said their investigations have shown that Speaker of Parliament Richard Msowoya, who was self-driving, was not in...
certificate bwana imeneyi nyumba yaku 43 ija munamanga nthaw yomweyi? munthu munamaliza school muli wankulu kale
Phwiyo repent and do an honest job.God will forgive you.Chuma cha umbanda sunapeze nacho mtendere.You wasted partying ndi ndalama za cashgate while a common Malawian was lacking essential services in healthcare.Kuombeledwa konsekuja anali matembelero.You were bringing bad karma to yourself.Mayi wako Joyce Banda amakuchemelera is not where to be seen.She is in her self imposed exile.Nayenso akuopa kuti azamuchosa masagwidi ndi zipolopolo.Malawians are very angry people with these cashgate issues.
Hm Pay Back Time!
Koma azimayi muli pa mavuto. Moti wina akumayitana achikulirewa kuti “Honey!!??” Kuopsa amwene kuli bwino nkhale mbeta.
Kapezeni ena mandala a mphwiyo. Ndikunyansa nkhopeko ndiye kungonyansiratu. Akazi anu sakuuzani?
577 BILLION woyeeee
Its better to live in a modest house built by your own money than living in a mansion full of issues.The man has lost all the respect.
He has money but no peace of mind.If he made money on his own through businesses he wouldn’t be going through all this.Look now some people in hospitals in Malawi died because of greediness of these people.Koma anthu timalangidwa pa dziko lapansi pompano.He no longer have respect for the money he spent on beer parties.
Mulibe ziwili passportzo?. Pajatu with money you can even have morethan 10 coppies of passports ku Malawi.
Pablus Secundulus mbava