Email a copy of 'Chakwera criticises ‘Mbofyo Mbofyo’ Malata and Cement Subsidy' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

61 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
fathi shehaab
8 years ago

kodi lsz wakutanini anthu inu…. he is doing his role very well indeed..he has well thought of ideas and he is not partizan thinker..check him out next 35yrs.. he id so relevant to mlw politics..dont try indimidate him….soopa mdima ayi ngakhale mphezi!

VICTOR
8 years ago

kachalichi komwe a Chakwera anali president kali ndi anthu ochepa ndichifukwa chake amalephera kulankhula zomveka. MCP ndichipani chachikulu tikupempha akulu akulu
monga achimango kuti munthuyu owononga chipani.zimene akukamba panozi zoti ife amcp tidzapanga zakuti zakuti izi zimapangidwa pa misonkhano yokopa anthu , osati ku nyumba yamalamulo. izi ndi zochititsa manyazi chipani chathu chokhazikikachi.What is happening now with Chakwera and jessie ,sizinachitikepo nthawi ya Kamuzu ,Chakwamba,ndi ATEMBO
CHOTSANI MUNTHUYU MUYIKE OYENERA

Kenkkk
Kenkkk
8 years ago

Levelheaded, that is utter nonsense. Typical dpp haters of mcp. The largest party or one with the largest majority in opposition always takes the lead in opposition and also seems to lead the whole opposition. He is the leader of mcp, the largest party in opposition and is actually considered as the opposition. Laz does not represent other opposition parties. He just happens to be the leader of mcp, the largest opposition party. Your suggestion is undemocratic and no where in the world do they follow such stupid suggestions. You want say the leader of the smallest party in opposition… Read more »

Hara Chrispine
Hara Chrispine
8 years ago

Kod Apa Zikugwirizana Bwanji Ndi Kugwa Mmanja Mwa Mulungu? I Hop My President Is Right And There Is No Any Mistake There. Try To Tell De Truth. Chakwera Will Rule This Country Come 2019

Isaac
Isaac
8 years ago

Chakwera should remember that chinthu choopsa ndiko kuchoka mdzanja lamulungu.And he should be reminded that he will not rule this country.

mache Joy
mache Joy
8 years ago

chala mwamba odi uko boma lili mmanja mwa petulo palibe wina wake kuchuluka nzeru

opharamutheko
opharamutheko
8 years ago

kkkkkkkk achakwera kushuka sikuyakhula zopanda mzeru zakozo.alwayz kumangotukwana bwanji if you have something to offer just say it to Malawi an.osati kumatinamiza kuti ukazalowa boma uzapanga zakuti ndizakuti shame on you.if you have something for us bwanji osatithandiza pakari pano pomwe tiri mavuto. songoleri opanda mzeru ife nanga tikafa 2019 isanafike uzalulira nd ani. ???? shame on yoouuu

changatengani
8 years ago

Asaaaa, Timalata tomalembana mwachinyengito? Za mkhutu.

Mapazi asiyana
Mapazi asiyana
8 years ago

Was he speaking as Leader of Opposition or MCP MP? Too much we jn MCP.

Decent Citizen
Decent Citizen
8 years ago

Chakwera is right and its only the Dpp illiterate dunderheads who cannot see any wrongs with their Malaya-cement subsidy.Malawi needs modern public building policy instead of waisting building some substandard houses in villages meant. for campaign.We need a well organised housing policy for the benefit of all Malawians not some some few individuals.Mu city kungodzaza tizinyumba tazidina apart from a few good looking houses built by owners who are busy wrestling with cashgate issues.This mbofyo mbofyo nyaphapi Pitala is leading us nowhere.

Read previous post:
Malawi Parliament delinks Lilongwe University from Aret, research station

Malawi Parliament on Wednesday delinked the Lilongwe University of Agriculture and Natural Resources (Luanar) from two scientific research stations. This...

Close