Email a copy of 'Chakwera holds MCP shadow cabinet meeting: Discuss Malawi situation' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

54 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
Nomvumeka
Nomvumeka
8 years ago

Ok

Noxy
9 years ago

Mtima suvala sanza

MAGEDE SIWANDALE
9 years ago

Ine ndikayankhulapo mumva eeh amakonda kwambiri apm ndiye chabwino tizisiye choncho sindilankhulapo kanthu paja ine siwandale

bentby smart
9 years ago

My beloved party

Tsikulokufa nyani.....

Kkkkkk! Wonders will never end. Tiyeni nazoni za u shadowzo

chakumanda betha
chakumanda betha
9 years ago

Vuto lathu ndi limeneli a Malawi kuvetsetsa zinthu kumativuta. Yanenedwa kuti shadow cabinet potengera anthu omwe alipo panopa munchipanimo. Mesa paja awiri sangayende limodzi asanapangane NDE anthu enawo kaya akumpoto kapena kumwera ayikidwamo bwanji poti ambiri mwa Iwo kamba ka dyera ndi kudzinva kaya kudzikonda ali otangwanika kufunafuna mpando kwa a pulezident a panowa. Koma akunama kuti afuna athandize boma mapulani NDE a Malawi tikufuna zomwezo tidzingonamizidyabe basis.. Chifukwa cha anthu ochepa ozindikira mwa umbuli ife mbuli kalefe tidzingotsatira poti tonse khungu likutivuta.. Kod munthu wosamudziwa ungachite naye zinthu zofanana..????

Katundumadzi
9 years ago

DPP ndi dilluuuuuu

jiks
9 years ago

Majoti will remain a life supporter of tha nyau party. Being one of the kangw’ingw’is gologolos will remain like that for life. Now that the party is being led by commander in chief of gule wamkulu, Lazaro. Tasiyani kuzipaka manyi kukamwa abale. Musamasanduke virombo muli anthu.

Majoti
Majoti
9 years ago

My Party For Life. Osati Nkhalamba Yopanda Mano Mkamwa, Kumangotafuna Lilime Nthawi Zonse!

pwt
pwt
9 years ago

mcp ndi yongoyerekeza mpaka kale, anthu akulu akulu nkumachita zongoyerekeza pali nzeru apa?

Read previous post:
Cama calls for boycott of South Africa’s outlets: ‘Black Friday’ in Malawi

The Consumers Association of Malawi (Cama) has condemned the xenophobic attacks of foreigners in South Africa including Malawians and has...

Close