iwe Wollkillima: ndiye ma team achisilikali muwaletse kumanyanso m’ma division. chifukwa akawina mu division azamenyabe super league. the best solution sikuthesa ma team a MDF, Koma ma civilian teams apeza ma sponsor kuti ma players asamathamangile ku ma team a MDF.
can’t blame the coach ,,,he was forced to work with the B team which is hard for any other coach ,,,let’s wait and see what will the new coach bring
Victor
8 years ago
On Red Lions, the coach has no problem but the problem came in when half of the main team was banned. The coach was to do with the second line imagine. This is the disease in football poor performance of players the coach pays.
Akulisinga
8 years ago
He has just been redeployed sill a man in uniform. prepare for DRC now.
WOIIKwilima
8 years ago
Ndidzakhala okondwa pakadzabwera Army Commander yemwe adzathetse matimu onse achisilikali nkupanga 3 army teams(chigawo chilichonse timu imodzi).Osati ngati mene zilili panozi & ngati sipakhala kusintha chaka cha m’mawa super league idzakhala ndi matimu 8 achisilikali representing 60% of super league teams zomwe sizidzakhala zopatsa ulemu. Kale m’mene kunali ma team atatu (Reds,Moyale&Mafco)achisilikali kunalibe udani pakati pa Army teams ndi civilian teams. Lero xBarracks vs dh mawa vBarracks vs G linali T vs KBarracks ife weekend iliyonse kumangomva Barracks vs ujeni aaaa khalangati tikumasowa zochita m’ma barracks mu bwanji chonsecho mutha kuyambitsa mipikisano yolimbilana nokha nokha m’ma barracks(eg tag of wars).… Read more »
Mzungumbuli
8 years ago
If it is not the requirement that the coach should be a ” a man in uniform” then you can just hire Peter Mgangira, former Siver Strickers midfielder azakuphunzitseni ” umodzi-umodzi” kkkkkkkkkkkkk.
Mc Dennis
8 years ago
Mmesa Munamutumiza Kunja Ku Belgum Ku Coaching Course Waipanso.Vuto Ndi Ban Yamapuleya Osati Coach.Chonchobe Zabwino Zonse New Coach
Thomas Bandah
8 years ago
Maybe The Management Has Thought It Wise To Fire The Coach.Lets Wait And See
iwe Wollkillima: ndiye ma team achisilikali muwaletse kumanyanso m’ma division. chifukwa akawina mu division azamenyabe super league. the best solution sikuthesa ma team a MDF, Koma ma civilian teams apeza ma sponsor kuti ma players asamathamangile ku ma team a MDF.
what about Mzuni fc, akutani Coach wanu ???
can’t blame the coach ,,,he was forced to work with the B team which is hard for any other coach ,,,let’s wait and see what will the new coach bring
On Red Lions, the coach has no problem but the problem came in when half of the main team was banned. The coach was to do with the second line imagine. This is the disease in football poor performance of players the coach pays.
He has just been redeployed sill a man in uniform. prepare for DRC now.
Ndidzakhala okondwa pakadzabwera Army Commander yemwe adzathetse matimu onse achisilikali nkupanga 3 army teams(chigawo chilichonse timu imodzi).Osati ngati mene zilili panozi & ngati sipakhala kusintha chaka cha m’mawa super league idzakhala ndi matimu 8 achisilikali representing 60% of super league teams zomwe sizidzakhala zopatsa ulemu. Kale m’mene kunali ma team atatu (Reds,Moyale&Mafco)achisilikali kunalibe udani pakati pa Army teams ndi civilian teams. Lero xBarracks vs dh mawa vBarracks vs G linali T vs KBarracks ife weekend iliyonse kumangomva Barracks vs ujeni aaaa khalangati tikumasowa zochita m’ma barracks mu bwanji chonsecho mutha kuyambitsa mipikisano yolimbilana nokha nokha m’ma barracks(eg tag of wars).… Read more »
If it is not the requirement that the coach should be a ” a man in uniform” then you can just hire Peter Mgangira, former Siver Strickers midfielder azakuphunzitseni ” umodzi-umodzi” kkkkkkkkkkkkk.
Mmesa Munamutumiza Kunja Ku Belgum Ku Coaching Course Waipanso.Vuto Ndi Ban Yamapuleya Osati Coach.Chonchobe Zabwino Zonse New Coach
Maybe The Management Has Thought It Wise To Fire The Coach.Lets Wait And See