Email a copy of 'Court grants lawyer bail: Mulemba involved in K50m Malawi cashgate' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

30 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
che
che
9 years ago

Tsiku anaomberedwa mphwiyo akulu awa sanagone kusamutsa ‘akatundu’ kunyumba kwa mphwiyo…otiuza kukhala mkazi wawo…ndipo on that day they met mphwiyo at Lounge Onthambi, nde amene mukuti mkulu ndiofatsa mungokamba ma style akabedwe and washing the money thru Knight & Knight amapanga ndiyeyu…azathu aku FDH Bank anatiuza kale kuti account ya Knight kumalowa ndalana zodabwitsa zedi…lets wait & see!

che
che
9 years ago

Mulungu oweruza aweruze basi…anthu oyipa inu osauka kumafa mzipatala inu mukudya kashi ya boma muli pheee…yakwana nthawi musova!

Achimidzimidzi
Achimidzimidzi
9 years ago

Head spinning! The hunters have been hunted mphakana khola.

Zagwa
Zagwa
9 years ago

Yambani siwakuba chabwino, ndi wa money laundering! “For now”

Aganya
Aganya
9 years ago

Yambani kaya si wakuba kaya chani, koma na apa anaba. Chomwe amati khikhikhi ndi mphwiyo nchani, amadziwa kuti adyapo. Amalandila zingati to acquire all these properties within 5 years isaa. Mukumuyikila kumbyoni ndi amene mukamupempha amakugayilani,

Sindi
Sindi
9 years ago

Joe and Max lawyers also facilitated the same for the owner of the Matindi. Money was from Lutepo to Mserembo through the law firm. He bough a mansion kwa Bvumbwe. Are you ACB going to arrest the lawyers too?

Jihad John
9 years ago

Head of crooks is Ralph Kasambara. Lawyers are struggling these days.

Independent Thinker
9 years ago

Amangidwe basi anthu akuba amenewa

ENOCK ALIMOYO
ENOCK ALIMOYO
9 years ago

LET JUSTICE PREVAIL

Mmodziyekha
9 years ago

Maloya ndi mkangowaona akudusa but now am getting the real picture!

Read previous post:
Airtel Malawi powers secondary school youth awards

In a bid to motivate and inspire academic excellence in young people, Airtel Malawi has pumped K2 million towards secondary...

Close