Email a copy of 'Court suspends Muluzi case: Malawi ex-president lawyer argues charges were ‘politically motivated’' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

29 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
chalera M.
9 years ago

Mulekeni Dr Muluzi kumunzunza pankhani yandale ayi,Muluzi is the best president ever ever Malawi had

yemweuja
yemweuja
9 years ago

u r talking about Muluzi nanga Bingu anaba zingati nanga JB komaso iweyo Peter ukuba zingati. Musayalutse Malawi andale nonse pathako panu

Penjaninge
Penjaninge
9 years ago

Koma malawiyu..tinabadwiranji ife?

chosatheka
chosatheka
9 years ago

There goes my favourite president.!!!!!!!!!!!!!! mufune musafune, he was the best there ever was.

OMEGA BEMA
9 years ago

That is why muluzi akukondana ndi peter in order to gain favours

Imraan Sadick
9 years ago

Lawyer koma ameneyu
Atcheya Woyeeeeee

ELECTORATE MZIKA
9 years ago

Kodi anthu andale inu m’matitenga aMalawife ngati zitsiru zanu eti?And now how much of our tax money is Bakili going to get in damage and compensation.And very soon you tell us Atupele is minister of ….cum second vice president.Why fooling the entire Malawi nation on a fake case where yet Malawians are losing out? Uve ndithu.

ricky
ricky
9 years ago

if you want your sins tobe forgiven, 4giv others first.

Chemtukanika
Chemtukanika
9 years ago

Iwe wakutsona khutu ndiwe womvetsa chisoni kwambiri.Bwanji ukutukwana chikhalirenicho watchulanso Yehova.Iweyo ngati sunachite tchimo lina liri lonse ku ntchio.pabanja kapena mmudzi mwako,kweza chala mmwamba.Pamaso pa Mulungu tchimo ndi tchimo.Ndikukumbutse,watukwanatu apa.

GWERO PRISON
9 years ago

Wobera anthu wosauka nonse !!

Lawyer ndi judge wamkulu ndi
Mulungu NAMALENGA

Sangalalani kondwani ndi mahule anuwo

KOMA MUWONA CHIWELUZO CHA MULUNGU PANSI PANO KAPENA KUMWAMBA

Read previous post:
I’m ready to help Bullets –Msungama

Kondi Msungama, who has officially resigned as Big Bullets FC chairperson, has said he will be more than willing to...

Close