Email a copy of 'Dedza Young Soccer accuse traffic police of harassment' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Dedza Young Soccer accuse traffic police of harassment' to a friend
A wrangle over chieftaincy in Chipeni 2 Village, T/A M’bang’ombe in Lilongwe, Wednesday left 37-year-old man dead and over five...
Eish man, my ex, is another story she doesnt want 2 c me wth someone behind. C now she is calling, kaya!
Ngati lamulo limagwila kwa aliyense bwa inuyo apolice mumadzadzana mchigalimoto. Chanuchija ena mpaka kusowa pokhala kuima ku bumper. Yakumbuyo ija. Zoti inuso mukachita ngozi mupatsa bzy ma civilian kukunyamula mumaiwala. Demet
A Jegwe khalani ngati munthu oti nkalasi analowamo nokha mukuti mudapanga exceed ndi munthu mmodzi,ndiye kuphwanya lamuloko kaya.Kapena mwina malamulo sagwira ntchito kwa anthu ena,amachita kusankha?
Well done policemen! The bus was indeed overloaded.
Koma ikanakhala lorry yokutha ikanadutsa poti yanyamula stupid dpp supporters going to a stupid political rally by stupid peter mathanyula…
Mr. Millias Pofera Salambula Jegwe, that is not harassment it is called road safety. Its for the good of your players. Next time your management should look for better transport
My Friend Jegwe Just Forget This People And Appeal To Ur Official A Bigger Minbus Next Time, A 35seater Is Suitable For Ur Team
Nonsense! Just look at the rickety minibus when it was arriving at CIVO it was still overloaded.
Don’t break no rules and the police wont trouble you!
Mumatero atraffic kuvuta,koma zikanakhala ndalama akanadusa.Kuteroko DZ munaipasa madalitso nkupambana
I always recommend traffic police for doing their job, had it been a traffic saziwa ntchito yao bwenzi ngozi za mini bus zilipo za mbiri. Palibe nkhani apa wamva iwe Jegwe Pofera next time muzatenge ma highroof awiri nanga ma player 18 + ma official munapangadi EXCEED capacity ya mini bus.