Email a copy of 'Deputy speaker Chiwaya called ‘witch’: Malawi Police arrest woman over remarks' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

42 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
Judah
8 years ago

wages of voting witches in office

therere
therere
8 years ago

Patricia Kailati mukungoyang’ana mayiyu akumulanda chuma?

Poisson
Poisson
8 years ago

Clement Chiwaya is indeed a witch. Asakane ameneyu!

Mjomba Yusuf
Mjomba Yusuf
8 years ago

ha ha ha ha ha ha ha ha ha ha ha ha ha ha ha ha ha ha kungoti mzimaiyu ndi wa PP and nkhani imeneyi ndikuidziwa kwambiri.

Achiwaya si olakwa plus sakugwiritsa ntchito moipa udindo wawo

Dhola za malo amenewa anadya kalekale ndipo stain imeneyi palibe ali mbali yake mngakhale mwana wawo amene

kambwali
kambwali
8 years ago

zachamba eti palibe nkhani apa

Mfumu Michesi
Mfumu Michesi
8 years ago

Kungoti inu anthu aku Mangochi ndinu mbuzi zosamva, chifukwa ngati kuli munthu mmodzi amene alibe usogoleri kupunduka ndi mtima omwe ndiye Clement Chiwaya. Koma mumamuvotera munthu wankhanza ngati ameneyu. 2014 unapulumukira mkamwa mwambudzi ndipo mark my words 2019 ulendo wako wochoka ku Parliament ndiwomangamanga. Nkhanza ndi m nyumba momwe munthu ameneyu. Mangochi Central sinthani ndithu galu ameneyu asakupusiseninso kaya ndi nyanga olo mbuyache amazamubeleka uja azabwelenso koma pano pokha aziwe mphamvu za amphawife kuzera mu voti yathu. Kuba ndalama za nyumba ku Parliament osakukwana koma uli ndibenso malo amphawi. Anakutuma ndani kuti ugulise timalo tomwe unali nato tija..

moffat lungu
moffat lungu
8 years ago

Mr Chiwaya claims to be too powerful but not before God. He is taking advantage of his position to victimise the poor woman. Please magistrate make sure that the woman is compensated if justice is to prevail. The issue of names is invalid

timer
timer
8 years ago

palibe nkhani apa

Taweni
Taweni
8 years ago

A government of witches and zombies will always hide behind draconian laws when they know they are bewitching innocent citizens.

Citizen

Yanyamukaaaa!!!
Yanyamukaaaa!!!
8 years ago

Don’t ever say Chiwaya is one of most powerful politician in Mangochi rather say he is one of the oppressive politicians Mangochi has ever had. Sikuti anthu ndi opusa chifukwa choti ndi amphawi as per your thinking no. Kodi iweyo Chiwaya watukwana anthu angati pa Mangochi including mafumu even a T/A Mponda amene. I think enough is enough sopano and come 2019 nyanga zako zonse I swear sizigwiranso ntchito maumboni ake ndamenewa ndithudi.. Mulungu awamenyera nkhondoyi anthu ake ndipo 2019 Mangochi Central iwonako usogoleri wa chifundo ndi manyazi ndi anthu.

Read previous post:
Zomba teachers take BT Synod, Save the Children to task over unpaid allowances

Primary school teachers working in Zomba Rural have petitioned Blantyre Synod Education Department and Save the Children Malawi for not...

Close