Email a copy of 'DPP’s MP Bon Kalindo apologizes for abandoning constituents in Mulanje South' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'DPP’s MP Bon Kalindo apologizes for abandoning constituents in Mulanje South' to a friend
Livingstonia synod rebel clerk Chimwemwe Mhango on Sunday during his church sermon at Kanengo CCAP in Lilongwe emphatically pleaded with...
Lord have mercy!!!winiko ndithu kukhala mp…anthu aku mulanje bdinu openga…chibwana chimenechi musazapangeso mu 2019..nde chitsiru chimenechi ka loan kaja nde kungogula tima galimoto…anzanu amakhala ndi ma truck osati tomwe muli natotu..mukaluza 2019 tizakuthandizani chani gwape iwen ndalama zozionela mochedwa..pempho kwa H.E ameneyu osazayelekeza kumuika mu cabinet..ndi galang anthe
Inu kodi mwaiwala kuti ndiwamasewelo uyu nanu,sono iye akamapezeka kumuziko muno ntown azitisekesa ndani kakakakak masankhasankha anuwa nanu kakakaka
Masankhasankha munasankha kape wachimizimizi.Amangowona ngati kutulo kuti ndi mp.iye kwake ndi kulimbana ndi a zungu a ma estate kuti a choke.wawusilu inu uyu.
My question to winiko , where have u been ?
unfortunate to slash the whole area simply because of mere personal differences. Which ethics is being followed here!
MUNTHU WAKUDA SAMANGOVOMERA TCHIMO LAKE AMAFUNA AMUPAKE NZAKE IYE KU MTIMA KUTI MBEEEEEEE A WINIKO TANGOVOMERANI KUTI MAGALIMOTO OVUTA AJA SANGAFIKE KUMUDZI ADZIKHULA PANSI KKKKKKKKKKKKKKK
Mkulu uyu amandiipira nkhope bwanji
Now I understand the extent of Kalindo’s stupidity and emptiness….it is soooo deep…the guy is dull, very dull. So Vincent Wandale, the Supreme Leader of PLO was right….
Alomwe mavotera votera nanga ndi Winiko wu Mp.Alomwe ndi mbuli bwanji
Remember the people who voted for you Mr. Kalinde.