Email a copy of 'Exposed: KB kept vigil at Civo ahead of knock-out tie' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Exposed: KB kept vigil at Civo ahead of knock-out tie' to a friend
Tribal grouping, Mulhakho wa Alhomwe (MWA), which has step up preparations for its annual celebrations in October, will this Friday, September...
Ma allowance akamasowa timatelo.Nsilikali wanzelu amapanga create ntchito kuti ana apeze kanganyase.inu mmati atani.mzanu mmene yavutila ya Malawimu.
Kikikikkiki kodi mateam okhulupirira nyanga alipobe ku malawi kuno? ndiye munapindulanji? anzanu a noma ndiawo akuvutika kupereka MK250,000.00 kwa mai a ku balaka nkana analuza pa home ndi CIVO, mpake asilikali anazolowera molingana ndi ntchito yawo, koma zantchito ndi mpira ngosiyana, inunso pantchito simunafikepo, kukabwera nkhondo kumalawi kuno ndipomwe titazaziwe kuti mankhwala anu amagwira apo bii! muzingonyika. anzanu a Jesus as juju ali pa top with 35 points unbeaten pompo dii kikikikikikiki
If juju works in football Mozambique could hv bn winning Afcon
kuzolowela ntchito zolonderalonderazi basi, zausilu!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!
Musanamizane khini ilipo!!
So KB still believes in juju? It’s true that their moving away from Dedza had a traditional belief that Dedza Young Soccer uses juju? I think it’s a sign that they themselves use khini kkkkkk
Hahaha if Juju works then Malawi could’ve qualified for World Cup, won World Cup a couple of times, we should have a World player of the year- in other words what Pofera has said is true
Anapindulanji?
ngati anthu otiteteza amene akukhulupilila zinthu zopusa ngati za ufiti, dziko lathu lingatsogole? as i’ve said before, mfiti ikadzalenga mankhwala a AIDS or cancer, kapena ikadzatiwinitsa world cup or even africa cup of nations then i will believe. otherwise, it’s all stupid bush business to me. nyo!
kkkkkkkkkkiest koma ziliko