Email a copy of 'First Lady says ‘this is the year’ women should pray for Malawi: International Women’s Day 2015' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'First Lady says ‘this is the year’ women should pray for Malawi: International Women’s Day 2015' to a friend
Malawi’s former First Lady Callista Mutharika has urged women to be more prayerful and should shoulder responsibility of protecting and...
koma munthu ndiwovuta kweni kweni azimai eeh dangerous creatures
Koma Callista is very bitter with Gertrude Mutharika? Why did she not attend. Kunama kuti you were not invited? Do people invite kumapemphero? It was on Tv, Radio iwe umafuna Cha? Paja unkati Peter asakwatire ukudziwa kuti he was dating Gertrude eti? Evil woman, jealous!! Just accept kuti sanakukwatire iweyo mmene umafunira. No chokolo!! Support Gertrude Basi apo bi drop the Mutharika name, you are embarrassing the royal family by not attending her functions. Iwe nkumakachita preside over mapemphero enanso???? Same day???. Uhule eti?? Ukupikisana ndi nda I??
Why this dirty language abale? In fact, mapemphero awa ofunika Mai Getu pa national level, Callister ku Region 1, Sannil Dzimbiri/Anne Muluzi ku Region 2, Mai Chilima ku district A, Mai Malawezi ku district B, Mai Chihana ku district C, Mai Chakwela ku district D etc etc.
Zokhalira kunyoza fellow mai tiyeni tizitayile uko. Chonde
YES YOU ARE RIGHT ABOUT THOSE AZIBAMBO taziasiyani azimayi azimasuka pokambilana zawo amayi president wotu amafuna kufunsa anzawo zina ndi zina za m banja abambo kupanda manyazi..
Please tawauzani awa apeze tailor. Embroidery every outfit that’s a thing of the past. Kumbwambwana basi!
Where was Calister Muthalika and Annie Muluzi? Xfirst ladies affair
Kkkkkkkkkkkkk koma guys
Hehehe. 1 event two functions…….ina ya Madam Callista.
For the first time since 1964 a woman, Joyce Banda, became State President in 2012. In 2014 the overwhelming majority of women did not vote for their fellow woman to have a first 5-year term as president. Why? Yes there was cashgate during Joyce Banda’s rule but the party that won led by Peter Mutharika-DPP had brought Malawi to its knees by April 2012 when it was being led by the late Bingu wa Mutharika. So I still wonder why the majority of women did not support their fellow woman to continue as state president. It is a true fact… Read more »
Mwazilowetsa masewera I think malawians r tired wth motherhood issues mumangotiberapo ndalama kodi azimayiwo up to now azidikilabe mafumu kuti aziwathangitsa , chiefs got a lot to do in development osati zamimba zanuzo, kodi anapereka mimbawo amakhala ali kuti ? Kodi amakhala opanda plan
Komanso a First Lady osakwecheka awa ine sindinaone. Kodi ku state house kulibe rexona