Email a copy of 'Gwamba, Onesimus deny Chinga’s song: Salanje says ‘stop the hate’' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Gwamba, Onesimus deny Chinga’s song: Salanje says ‘stop the hate’' to a friend
Pharmanova Malawi Limited (PLM) which received Best Manufacturers Award at the 27th Malawi International Trade Fair, last year on Friday...
nkhani ndiyakuti akubanja yankhulanipo.nonse mwangoti ziii bwanji.eeeee mukufuna athu aphane Kaye?.chonde Steve spesho yankhulanipo
Munthu yemwe anali wotchuka ngati Grace sangamwalire ndi kuikidwa mmanda opanda autopsy. Kunamweka kuti anangoti mutu basi kukafika kuchipatala ali wamwalira:
1. Mutu paokha simatenda.
2. Mutu nthawi zambiri umakhala chizindikiro chabe kuti penapake mthupi la munthu pali vuto.
3. Ndi chifukwa ninji amzake a Grace Chinga komanso opemphera naye sanakhale ndi chidwi choti adziwe cheni-cheni chomwe chinamupha Grace.
Mafunso ambiri akufunsidwa ndipo anthu akulozana zala chifukwa chakusalabadiraku kapena kuwabisila aMalawi chomwe chinavuta. Chonde achibale a Grace thetsani mopokosowa ponenapo kanthu.
Munthuyu wafa ndi mavuto ake. Sizimayenda kunkhani za banja basi. Mufunse omwe amakhala naye pafupi.
Mxiew!!
Zonse aziwa ndi mulungu even tidandaule motani wapita basi ngati nthawi yake idakwana zachitika ndipo ngati nthawi yake idali isadakwane ndi mphavu ya ziwanda adzaweluza jah jah pa 18 march 2017
zonse adziwa ndi YEHOVA
Tamva zambiri zikukambidwa.Salanje iwe wemwe umaloza chala kwa azitumiki anzako, you blamed them, today you tell people kt asalozane zala chonsecho unayamba ndiwe, tsopano ife tigwire ziti???. Ine ndimakhulupilira kwambiri munyimbo zomwe wina angayimbe cos mumakhala msg yonse yomveka bwino. Grace anatukutsa single titled Ndzauula;ndinaimvera ndi ku mvetsera bwino bwino uthenga wanyimboyi ndipo choona chake ndikutha kuchiona through this song, ndipo ndilibenso nthawi yoti wina andinamizenso ndizina. Ambuye ndiye angaziwe kuweluza zonse osati Ine or wina aliyense.
Time will tell.No need for finger pointing!
osalozana zala apa ayi munali kuti nthawi imene iye amatha maga
zi kawili pano ndiye muoneke ngati anthu odziwa kutanthawuza koma kuli kuda kwa ntima wanu nenani zina osawononga nthawi kudanitsa ntundu wa amalawi konse komwe ali
malawi have rost one of good comporsor like chinga.ndizaulula whos will wromch,?Ambujepe waimanyilile.mpumule mumtendele ni abam jenu jangani ji koposhe.ps