Email a copy of 'Hail the pious Malawi Police IG: Muckraking extra' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Hail the pious Malawi Police IG: Muckraking extra' to a friend
“If a problem is fixable, then there is no need to worry; If it's not fixable, then there is no help...
I was conned by a police officer just last week! He reported to have located the whereabouts of my lost Samsung s4 mobile phone and that he needed transport to travel to the location where it was beeping. He got MK7,000 from me to cover his transport costs but has since not given feedback. Believe you me I have given him 7 days grace period after which I will take action.
Akuba ndi apolisi omwewa. Komabe pali ena owopa Mulungu. Mbamva siwonse ayi. Aneneri onyenga.
Dzonzi is the best IG mukhito anakhala IG anthu Ali ndizochita dziko lino pomwe pano anthu alibe chochita ulova osayamba nde musaone ngati akulephera poti wapephera asanapite Ku ntchito.kungofuna muikepo bwava pampandopa eti
Before that operation was conducted,most of hardcore crimminals were tiped off by the same police.That’s why anagwira anthu ambiri osalakwa.
Wapolice akasala anthamangitsa bwanji wakuba?
awa ntchito ya police siyawo, a real man of GOD pray and fast wakhoba?
The DPP led government has the capacity to deal with crime. Please APM do a proper soul searching. Do you need Mukhito at State House or Police????
It has to start with the Lowest ranking officer learning to appreciate h/er/is role as being: `the most valuable one’. This will come only with concerted civic education and serious efforts to address their daily NEEDS and a start @ providing their WANTS. The same goes for the civil servants.
ATSOGOLERI WATHU AKULAKWA KUMAZIKUNDIKIRA NDALAMA Zankhaninkhani pamene ma junior Staff ndalama pangono ngono !! MA ALLOWANCE NDE OSANENA NDIZIMENE ZIMAWAPSESA MIYOYO MA JUNIOR OMWE AMAGWIRA BNTCHITONSO KWAMBIRI !! NANGA KU U S A ZIMATERO ??? BWANJI OSACHITAPO BKANTHU KUNO KWATHU ???
Mbava ziri mpolisi mmomo, “the recent half a billion kwacha heist at the Standard Bank in Mzuzu was traced back to a police officer in Blantyre who has since been arrested.”