Email a copy of 'Hailstorm destroys over 50 houses in Lilongwe' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Hailstorm destroys over 50 houses in Lilongwe' to a friend
Malawi TNM Super League champions Big Bullets are on the verge of exorcising the ghost that has haunted them for...
Boma lipemphe ndalama ku NAC!a2wa athandizidwe.
PleaseNAC buy iron sheets and cementfor the affected houses.
At least Malawians will understand the underlying causes this time than giving the money to Alhomwe , NAC and BEAM
Sorie for that, its very painful indeed
Zomvetsa chisoni Amalawi ena osowa umunthu mukumapereka ndemanga zonena mtundu wa achewa. Ngozi zadzidzidzi zingafikire mtundu uliwonse mnthawi ya kusintha kwa nyengo ino. Kumbukani CHINDINDINDI ku Karonga.
All lives have been saved in this village of 400 inhabitants. Let us support them to rebuild their lives.
Achewa tisonkhe ndalama apa ngakhale kuti khisimisi yatipha kale.
Kodi abomawo achitapo chian kuambira tsiku la zovutal? Boma pangani mashawi osat kungogula galimoto za apolice ena akuzgwiritsa ntchito pokaba ndalama kubank,filling station nd malo ena,athandzeni amalawi anzathu mawa ndnu ma ps
Ndi udindo waboma kuchita kathu pamavuto ogwa mwadzidzidzi enawo pambuyo paboma.pepani amalawi azathu.koma tisalowetse ndale pothandiza chonde.
I am just coming from Msenda village on a Red Cross mission where relief items were distributed. Eeesh. The situation is very pathetic and it is raining cats and dogs. The people in this village are very hard working as evidenced by the number of houses built with burnt bricks and iron sheets. I was positively Surprised that many of them are women. I wish more well wishers can come to support these people.
Anybody can help them not only government. NGO’s and other Organasations shld take part.