Email a copy of 'High Court rebuffs Malawi Law Society on Salima- Lilongwe water project: Injunction refused' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'High Court rebuffs Malawi Law Society on Salima- Lilongwe water project: Injunction refused' to a friend
President Peter Mutharika has pledged never to leave out women in his government’s development agenda. He said he recognized the...
Koma umbuli ku Malawi utipweteketsa.Kutereku anthu ena sakudziwika chifukwa chofunira EIA?
What is the purpose of wasting money Environmental Impact Assessment when the contract is already issued to Simbi? It seems this Director of Environment Affairs is not professional, and cannot learn from the failed Nsanje Inland Port as Mozambique stopped the project because of failure to do the environmental impact assessment first.
The tribal thing aside, let’s understand what is in the US$500million package. Malawi has rarely gone into such gigantic loan and I cannot recall one myself but I know that I am not a repository. Let’s not be simplistic in our approach to public procurents. The other time I heard that Malawi’s external debt is pegged at US$1.9 trillion and then add $500m from one Project.
Eish koma mwanna, bomali likuyesetsa kuika chitukuko … Madzi ku LL from Salima ku BT from Likhubula, Kammwamba solar electricity, miseu etc… nde ena nkumatenga chiletso, mawa aziti “Boma lalephera lichoke” a Malawi munakhala bwanji?
kodi akulu inu simukuwona kuti kusiya njira zina zofunikira ndi njira yobera ndalama zaboma. Mukudziwa kuti boma linawononga ndalama zambiri ku Nsanje pano project imeneija sidzathekanso koma ena anadyapo ndalama . Kodi anthuni chilungamo mudzachidziwa liti? Sndaliwa anayambitsaa chitukuko akudziwa kuti sichifika kumapeto, ndipo so iwowo alipampando adzakhala anapita.
Malawi Law Society is one of the most useless organizations – its full of idiotic people and attention-seeker who think they know better than anyone else. Our country can never develop with such stupid mentality. Always trying to show they are the most educated. Lilongwe needs water NOW! So all these so-called lawyers should SHUT their mouths. NONSENSE!
Mukangosiya Malawi Law Society mmanja mwa Atu mbuka umangoziwiratu kuti yalakwa. Khumbo Soko and Michael Chipeta. We know the issue is not about water. Any Malawian including your fellow Tumbukas knows that Lilongwe is facing acute water problems. But you think you gonna get inot government by stopping the project. Atumbuka Munya.
That’s Malawi for you…shame…
Kodi ine ndimadabwa….anthu mu Lilongwe akubvutika kuti apeze madzi, koma mukuti iyayi tikatenge injuction….eeee muchite kaye social impact assessment, feasibility study, etc Kodi inu a law society bwanji osamataya nthawi yanu polimbana ndi zinthu ngati maphunziro amane sakulongosokawa (ma university athu ana amakakhala miyezi yambimbiri kunyumba inu muli mphee…osamatenga ziletso zoti ma sukulu asatsekedwe bwanji?!), ma elections akukanika ku Lilongwe’wa, mbabva za ma minister…..bwanji mumakonda kukhala busy kuletsa zinthu zoti zinthandiza wanthu….mumandikwiitsa bwanji
These MLS boys are Just childish and greedy…All we want is permanent water solution in Lilongwe…By the way,where are the Law Society guys when People are building houses around mountains and hills in our cities? Why are they not quizing the Mulanje water Project and numerous projects done by Mota Engil?
paja Malawi law society ndi chipaninso . sometimes ma law expert athu ndiopusa heavy.
plz plz never do that again