Amayi anthu anu amu chipani akuvutika kwambiri koma inu mungoyenda yenda simungawapase poyambila.Mukuthandiza osawuka koma osawuka ali tho muchipani chanucho.Anthu munangowanamiza ndizakuthandizani mpaka lero.Tingowawona pa reach and touch.
KANJANI
9 years ago
SATANA NDI ZIWANDA ZAKE.
Alungwana
9 years ago
Glory be to God! Mama JB, I hope you have alot to do than being a president!
Weniweni
9 years ago
Koma dzikoli, mama we love you
munthu
9 years ago
That’s mama.. May God bless you.. Amalawi tiwone tokha kuti mayi amayendesa bwino dzikoli than mdalayu.. In just few months ourcurrently has already started showing signs of collapse.. Malawians will soon go into regrets…
Kika kanawe
9 years ago
Bravo!Amayi koma phuma musiye muzidekhanso ngati mmayi.
OUR FRIENDS NEED INTERNATIONAL AIRPORT; INTERNATIONAL STADIUM AND GOOD INFRASTRUCTURES IN THE NORTH PLEASE !! LETS HELP THEM 50 YEARS HAVE GONE DOWN THE DRAIN WITH NOTHING WORTH MENTIONING THERE !!!
Thoko
9 years ago
Nanga Aja Amati mukuwatsatila Aja a kuti bwanji??? Anabwelako kale kale with nothing to show for. Dziko likuwakanika kuyendetsa. Things are going down hill very fast.
AJB, Zikuvuta kukuiwalani, ngakhale ndinu mzimayi,koma zimkadziwika kuti dziko liri ndi mtsogoleli osati ziriko lelozi
Amayi anthu anu amu chipani akuvutika kwambiri koma inu mungoyenda yenda simungawapase poyambila.Mukuthandiza osawuka koma osawuka ali tho muchipani chanucho.Anthu munangowanamiza ndizakuthandizani mpaka lero.Tingowawona pa reach and touch.
SATANA NDI ZIWANDA ZAKE.
Glory be to God! Mama JB, I hope you have alot to do than being a president!
Koma dzikoli, mama we love you
That’s mama.. May God bless you.. Amalawi tiwone tokha kuti mayi amayendesa bwino dzikoli than mdalayu.. In just few months ourcurrently has already started showing signs of collapse.. Malawians will soon go into regrets…
Bravo!Amayi koma phuma musiye muzidekhanso ngati mmayi.
Mama all the best and we know you deliver.
OUR FRIENDS NEED INTERNATIONAL AIRPORT; INTERNATIONAL STADIUM AND GOOD INFRASTRUCTURES IN THE NORTH PLEASE !! LETS HELP THEM 50 YEARS HAVE GONE DOWN THE DRAIN WITH NOTHING WORTH MENTIONING THERE !!!
Nanga Aja Amati mukuwatsatila Aja a kuti bwanji??? Anabwelako kale kale with nothing to show for. Dziko likuwakanika kuyendetsa. Things are going down hill very fast.