Email a copy of 'Ibra Mwase laid to rest: Malawi ex-footballer' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Ibra Mwase laid to rest: Malawi ex-footballer' to a friend
Government through the Ministry of Agriculture and Food Security says it is intensifying irrigation farming in the country in order...
remember the song by dizzy manjeku and his papa disco Ibrahim in short ” ibra” The late Ibra was famous in football around that time. the late mwala moyo used to play that song i think in praise of Ibras achievements in football R.i.p
IBRA he was my f player.May your Soul Rest in Peace.
it is very unfortunate that people are talking alot now about ibra,to say the truth ibra was agood guy who used to mix with people during his pick.koma wakhala akuvutika palibe ndimodzi yemwe amene anamthandiza mpaka munthu kulowa ntchito ya uguard koma enanu osamukumbukira.zamanyazi
To all reporters in Malawi, you should stop reporting on issues without showing the real pictures. If Ibra was a great footballer, indeen he was, then you were supposed to show his pictures to the nation so that people could have the actual picture now in mind, You must not report for the sake of showbiz. Respect your job then people out there will respect you fake Malawi Reporters..
Rest in Peace Ibra, You were such inspiring player how Iremember as 10 year olds at Nyambadwe ground in the 1970s you could dribble past us as if you were born with a ball in your feet. I remember on those o’le innocent good days our rival teams always used to say “Ngati mukufuna kusewera ndi ife Ibra asalowe’ for nothing else but fearing your magic legs which always put off the rest of us no wonder you reached that far.May the Almighty cherish this time RIP Ibra.till we meet again in the Kingdom of God
RIP
remind us his time action, tidali ana
Inu a number 15 musasokez anthu a Mulungu pomanama ndikuphunzitsa za anthu akufa kutu Mulungu awalitse maso awo kuti awale kosatha. Simuwerenga baibulo kodi kut akufa sadziwa kanthu bi! ndipo kuti atsikila kuli chete! Tasiyani kungomvetsera zokuwerengerani mu Chitsime, tamawerengani baibulo yomwe it is entitled kuti “BUKHU LOPATULIKA NDIRO MAU A MULUNGU” osati la Malemba Oyera, ndilo muli ziphunzitso zabodzazo.
Inu a Nsembe tamawaphunzitsani chilungamo anthu ophunzira bwinobwinowa koma wosatha kuwerenga ndikumvetsetsa chomwe baibulo imanena za anthu akufa. Mulungutu akukuonani anthu mukuwasokezawa.
I agree with Mungete. Nanga nthawi zonse kuthamangira kuonetsa nkhope za anamalira phindu lake ndi liti? Kumbutsani anthu omwe anaiwala womwalira ndi zithunzi zake nthawi akali moyo kaya. Vuto lina ndi a FAM. Kodi muli nayo nkhokwe ya zithunzi za onse ochita masewera ngati a mpira? Please its time kumapanga za masiku ano zotukuka bwenzi tikumapumila zinthunzi za maukwati a chaka ndi chakawa nanga si tizingokhalira nkhani ndi zithuzi za umaliseche wa anthu ali ndi moyo okhaokh. I am 49 years, heard and praised Ibra a thousand times but I don’t remember to have met him. Ndine wa m’tauni ya… Read more »
Oh what a loss my teamate ’88. East and central Malawi team, very humble,respectiful,competitive,coach’s player and very friendly.RIP.