Email a copy of 'Is DPP government punishing Malawians?' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

34 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
Benson T Phiri
Benson T Phiri
8 years ago

Cool down GOD is in Control

nyekhu wa nyekhulani
nyekhu wa nyekhulani
8 years ago

kaya amwene

Kabalide
Kabalide
8 years ago

Ukanakhala ulaliki tikanangoti Amem!
Tikupita kuti?

ben matemba//chiradzulu

number 30 ayi mwaonjeza. mulungu akuona sikufunika kutukwana ayi, tikhululupile mulungu atisovela vuto lilipoli. Nanu atati che muthalika , tapanganipo kanthu mwachangu ,taonani mutowalakwitsa anthu potukwana, ngati zakukanikani nenani mwansnga kwa azipani zina kuti akunthandizeni, sikuti mutulepansi udindo ai koma mugwilane manja ndi opposition parties, apo bii ambwiye nditoona namutothamangisidwapo ,, khaleekhale anthu akutopelani ndinthu, aloma ndi achawa akangoyambapo kunongonezana ,,, hgozi, musazati ndi Che Chakwera. iwo angokhala kudikila mpando wawowo kuti muchokepo iwo akhale,,,, mapwiya tinene apa mpandowo ndi waeni,,,,,vuto ,,,zambiri mwanduna zanu makani ndi mwano,, kaya mumadziwaaaaa,,,,anthu alusatu moya,,,, angodikila nthawi ,,viva MCP VIVA TAMBALA WAKUDA

malawian
malawian
8 years ago

Nyani ameneyu akufuna kutimaliza, galu bwake nyani! cilibe umunthu cimeneci! kukamwa kwa kukulukuja! zoona anthu 115 yet developed countries took less than that! kuphunzira ndi kuendetsa dziko are 2 different! Mulungu kumwambako tithandizeni ndithu munthu ameneyu watikanika Ambuye!

Ch . Williams
8 years ago

Oooo God in the heaven hear our cry coz we are still in dark of bad omen, nakha zikuchitikazi ndi chan amalawi anzanga ndi liti lomwe tizasangalare eeeish.

fum
fum
8 years ago

Munthu wasala madzi amodzi mukuti alamulila mpaka 2019-dark cloud about to cover malawi soon or later

Sapitwa
Sapitwa
8 years ago

Things will get worse before they get better. We always complain as if we are an economic Island. Anzathu ngakhale ku Zambia alibe magetsi okwanira citing low water levels at Lake Kariba. Even the Zambia Kwacha is nose diving badly and yet they have mining! Malawians are a nation of complaints and crying just at nothing! You have to face the reality because thinking if impeaching the President on economic hardships can not happen and will not happen. He is President until 2019 hate him or love him! He can also win again if voting will be on tribal/ Regional… Read more »

kondwani
kondwani
8 years ago

Paja musayiwale ambendela analengeza utsiku bola akanalengeza masana chifukwa president tinamupeza utsiku we all still sleeping including the president amabungwe muli kuti koma zomwe zikuchitika ku chipatala mukuziwona? Muzalankhula ovata onse tikazamwalila? Ife anthu aku mudzi tilibe mkuwo tikudalira inu tithandizeni

clement
clement
8 years ago

Tiresome people. What do you want from the president?? To turn things for good needs everyone to do something not just looking at the govt to do miracles never happen. You must know that the president you are insulting will rule for the second term no fwifwi and DPP will be rulling beyond 2024 after prof Peter terms.

Read previous post:
Mutharika to discuss with Cabinet on Sustainable Development Goals

President Peter Mutharika said he will soon be discussing with his cabinet on how best to execute the 17 newly...

Close