Email a copy of 'It’s Mighty Be Forward Wanderers, K70m deal for Malawi football giants' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

56 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
mphatso
mphatso
9 years ago

timatimu ta kwathu ka club house ngati garage

clement
clement
9 years ago

Mine is just congrats To Be Forward for your rescue and my appeal to Wandereres management to use the finance suport properly.Lastly,its a request to the govt.WE need stadium in South pliz.

wakumozambique
wakumozambique
9 years ago

Nayo bullets yapeza sponsor wawo it wl be cald ‘rangers security bullets’logo yawo ndimutu wagalu

kumbu
kumbu
9 years ago

Proud of u manoma!!!!!!!!!!!!!

Prescott gonani junior

Manoma thandizo mwaalandila koma muchepese kusolola

princesaidmartin
princesaidmartin
9 years ago

manoma ndi deal

Oluza ali m'boma
Oluza ali m'boma
9 years ago

Tsopano ndipofunikira kuganizira aneba, ngakhale Boma lithe kulowelerapo, tangoganizirani ,ku Lilongwe : Silver,Civo ,Blue Eagles ,Kamuzu Barracks, Mafco ,Ma team othandizidwa ndi Boma okhaokha,komanso ma Studium atatu sopano Silver , Civo ndi likumangidwa kumene lija, pamena ku BTz kulibe team yothandizidwa ndi Boma kupatula mikango yaku Eastern Region, Kunena za Stadium ndi ija Mayi wamatewe uja, ndinena mbava yayikuluyi,ndinena Mayi uja analuza ali m’bomayu , unu ujayu, analandisa Stadium kuno ku mwerayu kutisiya pa mbalambanda opanda Stadium ati koma nkumafuna kuti tivotere ife aku mwera. Zausiru

m'bantu
9 years ago

usova wekha ndi kumwera kwakoko. kwa ife pa kapitolo,inde, LL, mayi ukunenayu ndi nyatwa. capital ikukongolerakongolera ndi chi stadium nyatwa, nyanga chikati chatha, u wil never taste an international match in the south,pepani.

Oluza ali m'boma
Oluza ali m'boma
9 years ago
Reply to  m'bantu

Mphwanga DPP ndi deal, imanga Stadium kawawa kuno ku Malawi, kaya zako izo ndi Matiki Chakwera wakoyo , m’busa wa feki

Jackson D. Ngumbi
9 years ago

Am a BB fan, but lets congratulate our friends for making it. Its not easy as we all conpeted for it. Lets pray for rest to hav also sponsorship.

Gerry
Gerry
9 years ago

Apa ndie manoma aiphulatu. congrats!!!!!!!!!

Joseph mbewe zomba
9 years ago

Sound gud 4 me

Read previous post:
TNM supports debate on financial sector laws: Donates K1m to Malawi Law Society for symposium

Premier mobile phone company TNM has donated K1 million to Malawi Law Society (MLS) as contribution towards a symposium on...

Close