Email a copy of 'Joyce Banda attacks ‘deeply corrupt’ DPP govt: ‘I’m coming back to Malawi, come what may’' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

61 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
Masopsu
Masopsu
7 years ago

bwera tikukufuna kuno wakuba iwe. usayese tizakumvera chisoni. unaba zochuluka sitizakusiya iwe ndi roy chule wakoyo.amati kachale kwanu konko.

mbili ya bakha
mbili ya bakha
7 years ago

kodi nanga nkhani ku CIKANGAWA yogulitsa mitengo/matabwa ku ZAMBIA NDI MMWENYE uja .anthu ambili anacotsedwa ncito opanda malipilo utalanda company from that fella mtse……lo uja??????????????????? ana aathu azimai kulephera sukulu. amai abambo kulephera kusamala mabanja ao coz of your greed. imeneyi unangoipsatila kaamba atidye nao anangoikhalila yet umati kukamba zolemba anthu nchito. mwana wako ndi iwe munazuza anthu, mwaocha eskom kuti zacamba unacita zijaso. kazibwera tili ndi umboni ose bwera uone.abale tigwilane manja apa. kodi aliyese angoti poti ndinali ku abroad nde ndikhale plesident! ZACAMBA. BWERA UONE UESA A MALAWI ALI MOMMUJA HULE IWE, SITEPE NGATI N’GONA

samuel kachipanda
7 years ago

palibe chosintha oloko mutabwera abiti hamala,inuo ndi a pitala ndiye bola tizuzike ndi pitala yemweyu.

Chipapwiche Kajhalwiche
Chipapwiche Kajhalwiche
7 years ago

Iwe Abiti Ntila..nawenso wachonatu chifukwa cha cashgate. Kuba aMalawi anzanga. Yako ija yotakata…kkkkkkk

mbili ya bakha
mbili ya bakha
7 years ago

kodi azatani bakha uyu. ubwere ndi
-ndege yathu
-maina aamene anaombera mphwiyo paja ukawaziwa anyamata okamwera mowa ku Joni. ulendo ku ma Pub a Joni ndalama lolololo
-ndondomeko yomwe ukufuna azapange kuno koz u r just making noise. zumbwe
-kodi ana a MAKANYA unangonama cithandizo, sukuwathandiza coz of your greed. pakamwa ndi pa bomatu
> utazatofotkoza misonkho yathu komwe imapita

Mudzamva liti
Mudzamva liti
7 years ago

Matchona tatopa nawo

paul
paul
7 years ago

DR Moses Ku Central medical stores alipo mafia and giving contracts pa Buy Malawi Campaign to Malawi pharmacies opanda ODPP tendering, katundu is overbought and rotting in warehouses at Central medical stores,. Investigate Dr Moses ACB

Chipapwiche Kajhalwiche
Chipapwiche Kajhalwiche
7 years ago

Is Abiti Ntila on a self imposed exile or cashgate induced one? Kubha mayi uyu. Ufele konko wamva? Nthawi yako yotakata pa misonko yathu inapita. Go to hell and roast you mother and baroness of corruption.

zako izo
zako izo
7 years ago

Ndalama zakuthelani mukufuna muzabe zina pano mgodi ulimanja mwa anzanu kwanu kunatha mai

chemuyaya
chemuyaya
7 years ago

I have come to the conclusion that Dausi has only three or four verbs

Read previous post:
Mutharika appoints Escom board members: Economist Perks Ligoya is chair

President Peter Mutharika has appointed board members of the troubled Electricity Supply Corporation of Malawi (Escom) with economist Perks Ligoya...

Close