Email a copy of 'Kids for K150m cash ‘traders’ jailed in Malawi' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Kids for K150m cash ‘traders’ jailed in Malawi' to a friend
Malawi’s top envoy to Japan who also doubles as the country’s envoy to South Korea but resident in Tokyo, Major...
Ku Thyolo kumeneko.
Tenant amagona nkumalota 120 million? Eee akanatukuka modabwitsatu. Kenaka akanagulitsa akazi akeo kuti agule Namiyo village yonse awapirikisemo abalache asalemo ekha. Kuteroko akaona anthu a ma estate ali amenewa amagula anthu. sagula anthu ameneo chifukwa chake anakatenga mphawi iwe kuti,uzialimira atukuke nawe ugulr wayilesi uzikasokosa nao ukanka kumuzi
Zodziyamba dala akuchepetserani zakazo kuli
Bwimo aknati mukakhale mukunyauda kundende moyo wanu wonse akhwrintotonu.
that’s killing deserve death sentence
Chilango chachepa apa¤
Matenanti Afodyanu,achewanu Ndinu Anthu Owopya Kwambiri. Fodya Mutibele,mwakwatiranso Our Sisters,mumawabeleketsa Ana Chaka Ndi Chaka,without Kulera,kenaka Mwayamba Kugulitsa Ana Ngati Mbuzi.Stupid,you Deserve Death Penalty!!
winawu siumphawi okha koma uchitsiru. Just imagine kumatengela za maiko ena nkumapha ma albino kuti akagulise ziwalo zawo. No sense.
Nenani kuti atumbuka tiwone apa. Mwachoka uko kuyipitsa anzanu.
Such unhuman behaviour some. Animals we call people
teach them a lesson!