Email a copy of 'Lawyer Mulemba arrested over Malawi cashgate probe' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

85 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
Cocoon
Cocoon
9 years ago

That is why Malawi is the poorest country in the world because people are just too selfish, brainless. Most Lawyers in Malawi are thieves, there no Justice, they still money from their clients and backed up by so called Law Society. Palibe chabwino, Government ndii anthu onse okuba.

Angoni
Angoni
9 years ago

@ Lusaka Zambia comment 25, i mean analemela just after two years chimalizileni school. sikuti am talking za lero ayi. get me right. I know him and his mother too ku MHC zomba office . He is also my friend.

paul mphwiyo
paul mphwiyo
9 years ago

Yambani is my true friend.

Jihadi John
Jihadi John
9 years ago

We need sharia law in Malawi and thereafter behead ALL lawyers!!!

akatswiri
9 years ago

Yambani Mulemba is one of humble Lawyers in Lilongwe ndiye osamaonjezera nkhani kuti ikome,kodi inu mulibe anzanu omwe anamagidwapo?why are you trying to spoil others?Ngati simukudziwa zaYambani funsani ife ngakhale mukhoza kufunsa anthu amene amagwira naye ntchito,God is watching you anthu ajerasi,is this murder or money laundering?kodi nkhani ya 92 billion ili pati?nanga nkhani yachasowa ili pati?nanga yachanthunya ili pati?God is watching from the distance watch out.

Innocent Soul
Innocent Soul
9 years ago

I never thought that there are many haters like this out here. I bet most of you dont even kno a story about Yambani. an you say he finished school 2years ago! my foot! get your facts right. Who told you that he was even mentored by Ralph? hahahahah… koma anthu inu musandiseketsa…..

Lusaka Zambia
Lusaka Zambia
9 years ago

Knight @ 30
Musapake munthu wolakwa please. Yambani was Mphiwyo’s friend in LL where is it said that he was also Noel’s friend. Does working together mean anzanu ndiamodzi? Kufuna kuonongerana mbili chifukwa chama jealous basi…

Lusaka Zambia
Lusaka Zambia
9 years ago

No 21 Angoni. Tikuvomera Yambani ndi mzake wa Mphwiyo koma muzinena zoona chonde. Yambani anamaliza school two years ago are you sure? Inu nomwe mati Mayi ake angulira nyumba ku 47 inu nomwe ku 15 inu nomwe ku Chirimba kungofuna kukometsa nkhani koma muziziwa kuti ndi mwana wa nzanu. Waipa Yambani chifukwa wamangidwa ndiye muonjezere nkhani.? Yambani has always been a humble lawyer and kukhala mzake wa Mphiwyo si kulakwa. Kodi inu anxanu onse ndi abwino??????????????

Abiti Sipoko
Abiti Sipoko
9 years ago

Iwe Katakwe make wa Yambani zankhudza. Anthu adabwa kuti ali ndi chuma chambiri within a short time fiscal police igwirapo ntchito apa kkkkk

Mzomera
Mzomera
9 years ago

koma abale, ndikumanva chisoni kwambiri. Akazi ena mu Lilongwe anathamangitsa azimuna awo akuti ndi osauka powayerekeza ndi amuna ena ogwira ntchito m’boma kachizungu kake amvekere ‘I cant keep suffering in poverty, my husband is very irresponsible’. Pano ndikhulupilira awona tsopano kuti aja amanyengana nawo aja anali akuba ndalama, amapeza ma contract achinyengo m’bomamu. zachisoni lero akuchita bwino ndi aja anasiyana nawo aja.

Read previous post:
Malawi hit by a smooth criminal

It is a documented fact that some of the world’s great men and liberation heroes spent some time in jail...

Close