Email a copy of '‘Looterpol’ accuses State of using him: Malawi chief cashgater bitter' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

31 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
Josephs Sande wa kwa Goliati
Josephs Sande wa kwa Goliati
8 years ago

Seriously my gray matter is unable to swallow this. Lutepo remember u havn’t been stable from the begining, over-changing of statements. Anyway, c u afta 11 years.

Che Ngana
8 years ago

Kutereku Unkaona Ngati Ukatchula Za Joyce Boma Likutaya Kumalimbana Ndi Joyce.Iwe Nkhuku Eti.Boma La Dpp Tu Lilibe Naye Ntchito Amene Uja Akamangidwa Amangidwila Zake Osati Kuti Bola Likumulonda.Ma Style Anu Athumbusuka Lero Tiyeni Zitchulanani.Nanu A Joyce Mutengerepo Phunziro Vuto Locheza Ndi Ana Amakutola Uchitsiru Chonchi.

Peter Mathanyula
8 years ago

Akuba okhaokha kupititsana ku ndende.

Kevin jackson
Kevin jackson
8 years ago

Ma judge athu, kuweruza mwachindunji. Tiyeni nawo osawasiya ayi, ankayesa ndi masewera.

amina
8 years ago

Why did you accept to be used. Were you the only person within. Anthu ena kunalibe okuti akanawagwilitsa ntchito imeneyo if iweyo umawakonda nthawi imeneyo a Malawi. Munthu wophunzila ngati iwe sukanalola tha!!! half. Umadziwa kuti ukuvutitsa miyoyo yosalakhwa lero a Mbuye ayankha ndi la foti ili. Chowuluka chili chonse chidzatera iwe lero watera basi. Paja a Malawi timamva nkhwangwa ili pa mutu. Tiyeni nazo.

Mlauzi
Mlauzi
8 years ago

Uyu angolongolayu just keep him under lock and key. By the way I thought I heard that Mikuyu Prison was closed? Why send him there at all? Mukufuna muzimupatsa preferential treatment without any prying eyes. Why not incarcerate him at Zomba maximum prison or even Penu Prison in Nsanje?

Chinyanga
Chinyanga
8 years ago

The guy failed to play his cards well hence sticking to his “amandiyuza” syndrome & now he still tries to buy sympathy from the very same malawians he took advantage of. Mr Lutepo, I dont blame u, I dont even blame those whom u formed the looting team with neither do I blame the judicial system…..I just blame the BLAME itself for its existence. Hop its time to dance to the tune of your own music. How I wish i could see others of your calibar following u.

Commissioner of Truths
Commissioner of Truths
8 years ago

Lutepo. Where is this ape from? District?

Daniel Phiri
Daniel Phiri
8 years ago

This idiot is not showing any remorse

walero
walero
8 years ago

Za 92billion iwalani ndipo zisiyeni coz kunalibe this casgate.zikanakhala zoonadi nthawi imene kunatuluka nkhani imeneyi bwenzi JB atawamanga onse a app nkuwaponya mndende,tisaiwalenso kuti paja inali nthawi ya campaign.JB anangofuna kuipisa mbiri ya anzake poti yake inali itada kale.a Malawi anzanga cashgate ya 92billion njaboza kulibe sinachitike kafunseni a Reserve Bank akakuuzani ndanenazi.

Read previous post:
MCP ‘dissident’ Jumbe says can’t join DPP

Malawi Congress Party (MCP) lawmaker Felix Jumbe has said he is being deemed as party “dissident”, saying despite rank and...

Close