Email a copy of 'Lutepo’s wife, daughter risk arrest: DPP asks cashgate chief suspect to seal ‘deal’' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

69 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
adona kuseli
adona kuseli
9 years ago

Chuma chapadziko chodwedwa ndi njenjete..Koma kumwambako kudzala ntchito Kaya ndangodutsamo ine.

njovu njovu
9 years ago

koma abale inu kumadyerera ife kumasauka mulungu akukhululukireni

eric phiri
9 years ago

anyanya

Independent Diplomat
9 years ago

Kkkkkkk kkkkkkk JB is afraid of Lootepo. She knows that she is in water.

fedrevolution
fedrevolution
9 years ago

When a legal officer wants to ends like curtains they join the government which doesnot win cases

King Matope
King Matope
9 years ago

Mukuyenera kuchita khanthu mwachangu!

Sindi
Sindi
9 years ago

Nanga Mserembo anakatenanga chi thumba chama hundreds of million Kwa Lutepo through lawyers joe and max?

Munthu Wanzeru
Munthu Wanzeru
9 years ago

Abale, ndawerenga ma comment onse koma tiyeni tisamale. Vuto pa Malawi ndi umphawi ndipo ndi umphawi omwewu umene anthu akuba ndalama za boma amabweretsera ziphuphu komanso ngakhale kugula olemba nkhani kuti asokoneze a Malawi. KODI MUDZIWA BWANJI KUTI MUNTHU WALEMBA NKHANIYU WAGULIDWA NDI LUTEPE OLO LOYA WINA KUTI APEZE SYMPATHY KWA ANTHU NDIPONSO AKUSOKEONEZENI MITU. ABALE PA MALAWI NDI NDALAMA CHILI CHONSE CHINGATHE KUTHEKA, TIYENI TISAMALE NDI NKHANIZI.

M'Malawi weniweni
M'Malawi weniweni
9 years ago

Why force Lutepo to implicate JB? Witch hunting eti? What if she is innocent, will she still be implicated for the sake of Lutepo’s freedom? Say the truth and truth shall set you free!

Kanyimbi
Kanyimbi
9 years ago

Kodi osamukwenya Lutepoyo kuti aulule amene amamutuma? Zinazinso ndiye bola milandu ngati imeneyi aziweluza mafumu. Mpaka boma likusowa poyambira?

Read previous post:
CounterJab: Jogging Tembo’s memory as wrinkle appears in Mutharika’s anti-federalism  

Former leader of the Malawi Congress Party (MCP) John Tembo and Monsignor Boniface Tamani joined the federalism debate this past...

Close