Email a copy of 'Madonna ends Malawi visit after meeting father of adopted son' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

12 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
Simeon Nyapala
Simeon Nyapala
9 years ago

zoona zikuoneka kuti abomawa sakuonetsa kuti mavutowa atha kuwasova. Maunduna ambiri ali ndi anthu oti sakudziwa chimene akuchita.

Nankhoma
Nankhoma
9 years ago

Kukaona ndi mtima wa munthu chabe otherwise its by force nkhalambazo sozimadziwa kuti adoption ndi chani amvetsetseni

isaac banda
isaac banda
9 years ago

Madona ndi nyatwa mumafuna mutakhala inu

tatha
tatha
9 years ago

what about relatives of mercy? you didnt meet them

kombozo
kombozo
9 years ago

masosalawo ndiye alibwinotu.

young george
young george
9 years ago

ali nawo mwai poti anapeza omuthandza kulera mwana

Ichocho
Ichocho
9 years ago

Prophet ndiwachimidzi

Pastor nyalapa
Pastor nyalapa
9 years ago

Prophet ndiwe mbuzidi chotukwanira mchiyani pamenepa umafuna uli iwe ukusilira mwana akukula bwino iwe wakalamba sangakutenge ufa usanatchuke komanso ndi umphawi kumangotukwana basi kulira ndi mtimatu kumeneko

Time
Time
9 years ago
Reply to  Pastor nyalapa

Ndipo kukalamba kuli apo, mwnanso ndo gojo. Ngati anabeleka, ndekuti akuvutika kulela anawo.

Prophet
Prophet
9 years ago
Reply to  Pastor nyalapa

Pastor,not that am jealous of anybody but just think a child being called an orphan and still his father is alive.

mtima wa nyani
mtima wa nyani
9 years ago

zomwezi mpaka ma unifomu, koma a mw ndi anthu ovetsa cisoni,
muone mmene atakatile anthu kusolola,
koma ndithu mulibe manya zi kudikila munthu wa 50 yrs kudzakumangilani skool akamafa nkugudumuka pa stage inu muli timangiledi, kunjaku mmene akutisekera anthu azungu? a plesident kugawa ndalama kumbali mwacisisi pomwe skool zathu ana akuphuzila pa ntengo ,modotha ,hhhee koma za ndondoli.
ntila ni anjimile anakamuka zaoyamba zija lelo muone chief civo , ps a maunduna akamukepo ,mudzandiuza.
wankulu akakhala kuipoa imamuuza ndi mphepo. mau aakulutu awa. APM …..

Prophet
Prophet
9 years ago

Mrs. Madonna Yohane Banda kkkkkkinkiest.A Yohah nkozo wanu ndithu.

Read previous post:
Madonna plans to build more schools in Malawi 

US pop diva Madonna through her  Raising Malawi has promised to give  Malawi children a gift of education as on Sunday...

Close