Email a copy of 'Malawi army soldiers confront cops on patrol in Zomba' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

123 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
felix
felix
9 years ago

ngati zalakwika tikambiirane olakwa apepese

Chikasandungu
Chikasandungu
9 years ago

Basi guyz kambilanani zokulirana mitima sizabwino,nanunso apolice munzivetsa zinthu .sikuti mau ochokera mkamwamwanu nde abwino kuposa aliyese ayi,tiyakhulane mwabwinobwino.

yungsai
9 years ago

let’s kipon praying myb Allah can bless malawi than fighting each other,if you can follow what the holly books says that chamoyo chilichonse chidzafa then who are we to forget those words.ofcz ndizowawa ndimmene izi zachitikra koma tisanene kut pot wawombera ndi wapolice koma mukumbuke kut kupha ndi kwa Allah cz ndiyemwe analenga zabwino ndi zowawa.pepan anamalira nonse.

MPHEREMBE WARRIORS
MPHEREMBE WARRIORS
9 years ago

declare war btwn MDF and MPS

lindamadziapite
lindamadziapite
9 years ago

Mwakukoma mtima kwa Mulungu, anatimatsa mphatso ya moyo , ndipo Mulungu Mzimu woyera amatipatsa mphatso yanzeru zakuti titazigwiritsa bwino ntchito moyenera,ndimoopa Mulungu zonsezi tikumvazi ndi zinthu zopeweka. Abale athu a Army ndi Apolice ndi anthu amene ife monga nzika za dziko lino timadalira kumbali ya chitetezo. Koma chodabwitsa ndichakuti iwo monga ana amodzi, amakhala omakulirana mitima ndikumachitana chipongwe. Chimene inu abale athu muyenera kudziwa ndichakuti mutamagwira ntchito mwaumodzi, dziko lino likhoza kukhala ndi chitetezo chamvamvu. Nanga tsono mukayamba inuyo kufunirana zoipa kodi ife monga nzika zadziko lino tiphunzirapo chiyani kuntchito yabwino yotamandika yomwe inu munaphunzidwayi. Pempho kwa akulu akulu mbali… Read more »

ZONYONANA
9 years ago

I wonder are those plain clothed confronters really soldiers? Why not doing their stupidity while in their uniform?What were they afraid of?A true citizen cannot clap hands for the soldiers intimidating police officers on duty.This can lead to a lapse in internal security-thieves can be given full control and there can be day light robbery.Were the confronted Police officers really assured that the confronters were our beloved soldiers?I am afraid those guys could be an organised group disguising themselves as MDF.So our Police be on the watch.

soldier weniweni
9 years ago

ta army timadzifila ngati tigamenye. tikamaliza ka training kawo timangokhalira kugona mpaka retirement. apolice kukhala cheteku asaone ngati kupusa. akayamba kubwezera ta army tochepa kaleti ndiye titheratu. ta army-to tizisiyanisa POLICE ndi MYP. ti anyani tachabechabe. ta army USAVEGE unawachulukira. mxxx!

Sosten Gwengwe
Sosten Gwengwe
9 years ago

How come it’s only soldiers who are shot? Something must be wrong with them

Jimmy
9 years ago

Lack of civic education.Foolish & stupid behaviour of a small MDF towards MP.This is unacceptable and you can hardly see it happening in developed countries.What picture do u show to the public here.

Domie
Domie
9 years ago

Apolice Mwaonjeza,mpaka Kuchotsa Moyo? I think u must apologise

Read previous post:
MCP conceals its stand on federalism: Chakwera says no intimidation

President for Malawi’s leading opposition party in parliament MCP, Dr Lazarus Chakwera says his party is yet to make its...

Close