Email a copy of 'Malawi arrest 8 DRC rebels for illegal entry in Karonga' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Malawi arrest 8 DRC rebels for illegal entry in Karonga' to a friend
Malawi government has deployed military helicopters and boats to rescue flood victims but despite high waters in the lower shire...
If they are real assylum seekers amathawitanji
mmanja mwa a immigration? Mlandu umenewo, ndi mbava zomenezo. A court thanani nawo
Much as I respect human rights, koma apa we must trade carefully. Anthuwa afunsidwe mokwana bwino ndithu ndipo ngati ndikoenera abwezedwe ku DRC.
BBC wake up please. If and i repeat if at the end of the day these are a danger then send them back. As for Mwafulirwa the British are always gullible there is no FGM in Malawi. If she is a Lesbian who cares there are many of her type in malawi and there are not persecuted. Why should you be screaming am a lesbian? As for the Congolese i urge govt to be tough make malawi unattractive and like zambia the camp should be moved to Karonga and arrest any of them found in Lilongwe. In this country we… Read more »
Alufeyo I think you have lost your senses nkhani ili apa sikugwirizana ndimunthu wamutchula apayu kodi iwe ndiwe otani musiye munthu apume nkhani ili yonse ingatuluke ukumamutchula ndikukudziwatu bwanji ukuvala chigoma osabwera poyera udzaona polekera iwe komawe umakhala ndudziwako nditha kukulembera aganyu mbuzi yeniyeni nde iwe komwe uliko udziwe zimenezo.
Akufuna azibale awo ku north,ambiri kumeneko ndima congolize. akufuna kuwathandiza kuti ayime pawokha atumbuka!
Please these people the way i look at them they are not fighters but they are trying to gain refugee status in malawi in such away of puting themselve on the cross by lie .
These people are refugees dont misstreat them listen to their stories …and make decision based on the evidence then send them home or consider them.. we know somany congeleese holding our chiphaso in Europe or canada they came in that way …
Please send them back immediately we are sick and tired of hearing of Ashababu, Isis, Bokoharam .Let them continue their killing else where otherwise we don’t like violate pple
ASK UNITED NATIONS TO ASSIST YOU IN HANDLING THE GUYS, DO NOT RASH WITH THE RULING.
Let them go to their country, ayenda bwanji kuchokera ku congo adusa maiko angati kuti afike kuno ku malawi, kwinaku kulibe ma Refugee camp apite basi angangoyamba kutibweresera ibola amenewo and I want to ask a BBC PHIRI KUTI ARE YOU A CONGOLEESE chifukwa zimene wanena sizikugwirizana ndi nkhani imeneyi you are there kukamkumba Mwafulirwa ali ku UK what is your problem ngati umaziwa zambiri osangopitako bwanji naweso ndikukapanga zimene anachita mwafulirwayu , ngati umakhala mu dzikomo ngati refugee uziwe kuti uli ndi mwayi ozakhala dziko la mtendere ngati limenero. Zachamba eti unasowa nkhani, Nobody wants to hear about Mwafulirwa’s… Read more »
APHUNZITSE A DPP CADET KUMENYA NKHONDO IJA YA ZIKWANJE
I do believe what has been published…. These young men can not be M23 rebels. Come on Mr Policeman..they just need asylum seeker documents. Please make sure to verify any information before you pass it to the media.