Email a copy of 'Malawi bank robbery cop provided vehicle for the ‘hit’' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Malawi bank robbery cop provided vehicle for the ‘hit’' to a friend
Ebola outbreak in West Africa has cost Malawi the first ever show of the Jamaican reggae artist Luciano. According to...
How did he pass all those roadblocks between Blantyre and Mzuzu without anyone noticing it was a stolen car? Malawi never ceases to amaze me
Ntchito ya anthu a ku south. Like president, shupiti.
Malipiro awo ndi otchepa anthuwa. Kodi paja APM samati awaonjezera ndarama anthuwa, Dziri kuti nanga lero. A Police tiyeni tichite strike basi ndalama yathu ya pa mwezi ndiyochepesesa pa dziko lapasi pano
Ameneyi tamudziwa coz wagwidwa, meaning there are a bunch of them out there. Danger2!!!!!!
Jugment yake muzamvanso kut 3 yearz
Fake Police. A bunch of corrupt Crooks and Thieves.
Together with Your President and Home affairs Minister.
MXiiiiii
Amafunika Kuotchedwe Ameneyo
Why Police Officers are being involved in robbery? The reason is their monthly taking is not enough for them to earn a living. Please revise their salaries so that they should reduce being tempted. Just imagine a police office who is getting K45,000.00 as his/her monthly pay but he/she is guarding billions of monies so him/her not being tempted by these monies.
Choncho tikudalireni inu? mwatiwopsya kwambiri. zonsezi ndichifukwa chamalipiro ochepa. tawawonjezeraniko malipilowo adzisangalala kwinaku nkumatitetezazo.
Apatu palibe chitetezo. Palinso police pamenepa?
A makhoti chonde tithandizeni don’t give bail to this man as he is a threat to society. More over the right to bail is not absolute. A state nanu lowetsani nkhani mu court. What type of evidence are u stil looking for?