Email a copy of 'Malawi coach Mtawali refuses to guarantee Ng’ambi starting place' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Malawi coach Mtawali refuses to guarantee Ng’ambi starting place' to a friend
Malawi Congress Party (MCP) parliamentary leadership has delivered a stinging criticism to governing Democratic Progressive Party (DPP) led by Peter Mutharika...
Though perfomance is key wat Earnest has toked cant motivate Robert to play for flames, Managers in EPL, la Liga, Bunde they back players they tok gud about players just to motivate them.We nid combination of old and young guns Mbesuma in Zambia is still playing and he scored in similar competition. We nid Esau Ngambi and Fischer
Ine sindinawonepo kuti pamudzi amapha akuluakulu One nkumayembekezera kuti mudziwo uziyenda bwinobwino. Tiwonera inu a Mtawali ndithu.
kodi olo kochiwathuyu tinkamchemerera ali wosewera anapangapo chiyani olo ndi chikho chiti angaonese kuti anatengerapo?Pasani mwayi anzanu sanje ai,nanunso muna pasidwa mwayi muli kujoni mutatchona.
Enerst mtawali ali ndi masiku ochepa chifukwa akulimbana ndi ma players. Ndipo ali ndi nsanje chifukwa bagio akumenya mpira wabwino kuposa mmene enerst amameyra. Musiyeni timuwona. Amalawife sitichedwa kunyanyala. Kusiya bagio , kamwendo ndi mulandu wawukulu. Be ready to pack and go
bajio, kamwendo matama pa field, mbuli inu!! ur old nw & wi hven’t benefit anytin’ frm u. Tikufuna ana ife asewereko! Mtawali big up! Chose players frm de pitch osati chifukwa ndiwakale!
Who is supposed to eat a humble pie the performance of Ng’ambi today when his team Platinum Stars humiliated Supersport United 3-1 with him scoring a goal. He is a midfielder but look the way he scores in a competitive league like PSL.
Komatu baggio mukunyozayo, mukanakhala ngati wina, simunakamunyoza. Kodi Yaya Toure si uyooo adakari mpaka pano, kusewerera team ya ivorecost? Ali ndizaka zingati? Mmmnm, abalee” mtima wansanje muzasiya liti? NdichifukwA chaketu nthawi zina mulungu samakudalisani munyumba mwanu, chifukwa cha mtima wansanje….and his problem simdziwa kusewera mpira, and u like too mucj complain, shame on u. U must go to church sometimes, maybe, god can make favour u.
For a very long time I have been an admirer of Ntawali but now it seems that Mr Ntawali is losing it. Who needs the one most in between Ng’ambi & Flames?????? By the look of things Ng’ambi is a hot potato at his club Platinum Stars & he does need anything to prove to anyone. He bring paid handsomely in Rands with the current rate of R1-K40 does he need the Flames????? My guess NO but on the other hand as a nation we need a player of his calibre in our national team. So Mr Ntawali just try… Read more »
Kodi Ngambi wanuyo anayamba liti playing for Flames? Which trophy did he bring to Malawi? iyaaaa! shut up ! no wonder ma coach ena nkayitana ndi achina Kondowe in a competitive game ati Anong’a Anog’a zoona???? Agalu inu. Ngambi ndinayamba kumumva ine ndili primary longtime back and now he should be above 48 years koma age yaku RSA adakali 35 years shaaaa!!!
Yes Baggio is agud player but how many games did he play and Malawi bring atrophy ?even Cosafa cup.sometimes we don’t do well coz professionals guarantee themselves position.Coach do u r job let people talk.