Email a copy of 'Malawi College of Accountancy lecturer arrested over cashgate' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

21 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
ken
ken
8 years ago

ife tinathawa umphawi pano tili ku theba kugwira ntchito zomwe zikadatukula lathu dziko. kuzunzika. abale athu kumalawiko kumudziko tikufunako koma mantha atigwira ndizomwe zikunvekazi……… tidzingogwirabe ukayidiwu kuno.

mache Joy
mache Joy
8 years ago

Kodi azingomangidwa osalandidwa kena kake?? ali ndi chuma chambiri chooneka osatengako manyumba ndi ma house ooneka wa bwanji??? mcheew imandikweza dpp bwanji nkhani imeneyi kunali kungoauza apange surrender chumacho coz olo akasekeredwe 20years azidyabe money yakubayitu

ZABWEKA RU
8 years ago

muchimina

State Counsel
State Counsel
8 years ago

Why don’t you arrest Radison Mwadiwa- Former Secretary to the Treasury. Newby Kumwembe, Dalitso Kabambe, Charled Tchuka etc.

Amfumu
8 years ago

Nanga JOICE mummanga liti? Mukumamuwopa akafufuma.

Amfumu
8 years ago

don’t waste our time reading fake stories.kumangomanga anthu chifukwa chowawonerera. akuba eni eniwo mukuwawopa. za zii.

thako la mmwenye
thako la mmwenye
8 years ago

kodi inu a ACB mpongozi wawo wa a Lipenga aku mangochi kuno Alexander Makina yemwenso makolo ake amakhala konkuno, mfana oyipa wakuba bad mummanga liti. Poti iye ndi amene anali conduit pakati pa mphwiyo ndi amayi. kapenatu ingokhala mob justice- zimatiwawatu ife mafana amene aja akamanjoya ndi dollar yokuba ndikumaoneka ngati a mzeru heavy.

Issa Kabudula
Issa Kabudula
8 years ago

The fear I have is that the more Mphwiyo is pushed to the ground the more the top big guns will be apprehended. kwendenayo!!!!!!

o
o
8 years ago
Reply to  Issa Kabudula

So, why are your afraid? Are you one of them?

hyndee
hyndee
8 years ago

Mulopwana ndiwe galu. Ufa ndi umphawi.kadzidzi wachabechabe iwe.

mike
mike
8 years ago

wina aliyense ndimbava ku Malawi

Read previous post:
Campaign for Female Education in Malawi calls for change of mindset to keep girls in school

Campaign for Female Education (Camfed) in Malawi has indicated that although various organizations were coming up with interventions to help...

Close