Email a copy of 'Malawi expectant mom sues CCAP church for defamation' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Malawi expectant mom sues CCAP church for defamation' to a friend
President Peter Mutharika has stressed the important role good road networks play in sustainable economic development saying poor roads inhibit...
Sorry
# suicide bonza.leave sda alone,sin is sin.no church can condone that according to the teaching of the master Jesus.how can yu label another church for a particular sin and take yurself as holy.search yurself and repent.dont take what those reciting poetly says.
something happened, the church can not organise an iquiry pa zinthu zomwe sizoona
amayi ngati mumapemphera ndibwino kungogwada kwa mulungu wanu chifukwa mukalimbana ndianthu sizikunthandizani konse.these are endtimes coz munthu kutengera mpingo kukhoti ayi ndithu.
And the relevency of the picture being?
MA CHALICHI CHONDE MUZISATILANI DONGOTSOLO LA BWINO POCHITA ZITHU, OSATI KUPUPULUMA AYI, FUSA MALOWA ANU POYAMBA AKUTHANDIZENI.
chikumulimbitsa mtima mayiyu ndi mtsogoleri wotayikayu kuti apite ku court
Lord have mercy
chilipo chinachitika ndi mtsogoleri ameneyu atsogoleri sangangomuganizira ayi,mkuluwampingoyu mkutheka anadya mayiyu.koma kuti manasoweka mzeru ndipopita kukafufuza kwa mayiyu amene si membara wa CCAP.koma izi sizachilendo azitsogoleri ambiri akudyerera azimayi mwa mseri ena mpakana mahule akumadya ndithu.Ambuye atithandiz
Church elders please do your own business look Now who wil Pay the Price??